Salimo 2
1Nʼchifukwa chiyani anthu a mitundu ina akufuna kuchita chiwembu?
Akonzekeranji zopanda pake anthu?
2Mafumu a dziko lapansi akugwirizana nazo;
ndipo olamulira asonkhana pamodzi
kulimbana ndi Ambuye
ndi wodzozedwa wakeyo.
3Iwo akunena kuti, “Tiyeni timasule magoli awo
ndipo titaye zingwe zawo.”
4Wokhala mmwamba akuseka;
Ambuye akuwanyoza iwowo.
5Ndipo iye awadzudzula mu mkwiyo wake
ndi kuwaopseza mu ukali wake, kunena kuti,
6“Ine ndakhazikitsa mfumu yanga
pa Ziyoni, phiri langa loyera.”
7Ine ndidzalengeza zimene Yehova walamula:
Iye anati kwa Ine, “Iwe ndiwe mwana wanga;
lero Ine ndakhala Atate ako.
8Tandipempha,
ndipo ndidzachititsa kuti mitundu ya anthu ikhale cholowa chako;
malekezero a dziko lapansi kuti akhale chuma chako.
9Iweyo udzawalamulira ndi ndodo yaufumu yachitsulo;
udzawaphwanya zidutswazidutswa ngati zowumba zadothi.”
10Kotero, inu mafumu, chenjerani;
chenjezedwani, inu olamulira a dziko lapansi.
11Tumikirani Yehova mwa mantha
ndi kukondwerera ulamuliro wake monjenjemera.
12Mpsopsoneni mwanayo kuti angakwiye;
kuti mungawonongedwe mʼnjira zanu,
pakuti ukali wake utha kuuka mʼkanthawi kochepa.
Odala ndi onse amene amathawira kwa Iye.
Salmo 2
1Por que se amotinam2.1 A Septuaginta diz se enfurecem. as nações
e os povos tramam em vão?
2Os reis da terra tomam posição
e os governantes conspiram unidos
contra o Senhor e contra o seu ungido, e dizem:
3“Façamos em pedaços as suas correntes,
lancemos de nós as suas algemas!”
4Do seu trono nos céus
o Senhor põe-se a rir e caçoa deles.
5Em sua ira os repreende
e em seu furor os aterroriza, dizendo:
6“Eu mesmo estabeleci o meu rei
em Sião, no meu santo monte”.
7Proclamarei o decreto do Senhor:
Ele me disse: “Tu és meu filho;
eu hoje te gerei.
8Pede-me, e te darei as nações como herança
e os confins da terra como tua propriedade.
9Tu as quebrarás com vara de ferro2.9 Ou as governarás com cetro de ferro
e as despedaçarás como a um vaso de barro”.
10Por isso, ó reis, sejam prudentes;
aceitem a advertência, autoridades da terra.
11Adorem o Senhor com temor;
exultem com tremor.
12Beijem o filho,2.12 Os versículos 11 e 12 permitem traduções alternativas. para que ele não se ire
e vocês não sejam destruídos de repente,
pois num instante acende-se a sua ira.
Como são felizes todos os que nele se refugiam!