Masalimo 2 – CCL & LCB

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Masalimo 2:1-12

Salimo 2

1Nʼchifukwa chiyani anthu a mitundu ina akufuna kuchita chiwembu?

Akonzekeranji zopanda pake anthu?

2Mafumu a dziko lapansi akugwirizana nazo;

ndipo olamulira asonkhana pamodzi

kulimbana ndi Ambuye

ndi wodzozedwa wakeyo.

3Iwo akunena kuti, “Tiyeni timasule magoli awo

ndipo titaye zingwe zawo.”

4Wokhala mmwamba akuseka;

Ambuye akuwanyoza iwowo.

5Ndipo iye awadzudzula mu mkwiyo wake

ndi kuwaopseza mu ukali wake, kunena kuti,

6“Ine ndakhazikitsa mfumu yanga

pa Ziyoni, phiri langa loyera.”

7Ine ndidzalengeza zimene Yehova walamula:

Iye anati kwa Ine, “Iwe ndiwe mwana wanga;

lero Ine ndakhala Atate ako.

8Tandipempha,

ndipo ndidzachititsa kuti mitundu ya anthu ikhale cholowa chako;

malekezero a dziko lapansi kuti akhale chuma chako.

9Iweyo udzawalamulira ndi ndodo yaufumu yachitsulo;

udzawaphwanya zidutswazidutswa ngati zowumba zadothi.”

10Kotero, inu mafumu, chenjerani;

chenjezedwani, inu olamulira a dziko lapansi.

11Tumikirani Yehova mwa mantha

ndi kukondwerera ulamuliro wake monjenjemera.

12Mpsopsoneni mwanayo kuti angakwiye;

kuti mungawonongedwe mʼnjira zanu,

pakuti ukali wake utha kuuka mʼkanthawi kochepa.

Odala ndi onse amene amathawira kwa Iye.

Luganda Contemporary Bible

Zabbuli 2:1-12

Zabbuli 2

12:1 Zab 21:11Lwaki amawanga geegugunga

n’abantu ne bateganira obwereere okusala enkwe?

22:2 a Zab 48:4 b Zab 74:18, 23; Yk 1:41; Bik 4:25-26*Bakabaka ab’ensi bakuŋŋaanye,

n’abafuzi ne bateeseza wamu

ku Mukama

ne ku Kristo we, nga bagamba nti,

32:3 Yer 5:5“Ka tukutule enjegere zaabwe,

era tweyambulemu ekikoligo kyabwe.”

42:4 Zab 37:13; 59:8; Nge 1:26Naye Katonda oyo atuula mu ggulu,

abasekerera busekerezi, n’enkwe zaabwe ezitaliimu zimusesa.

52:5 Zab 21:9; 78:49-50N’alyoka abanenya ng’ajjudde obusungu,

n’abatiisa nnyo ng’aswakidde.

6N’abagamba nti, “Ddala ddala nateekawo kabaka owange

ku lusozi lwange Sayuuni olutukuvu.”

72:7 Bik 13:33*; Beb 1:5*Nzija kulangirira ekiragiro kya Mukama:

kubanga yaŋŋamba nti, “Ggwe oli Mwana wange,

olwa leero nfuuse kitaawo.

82:8 Zab 22:27Nsaba,

nange ndikuwa amawanga gonna okuba obusika bwo,

era n’ensi yonna gy’ekoma okuba amatwale go.

92:9 a Kub 12:5 b Zab 89:23 c Kub 2:27*Olibafugisa omuggo ogw’ekyuma,

era olibabetenta ng’entamu y’omubumbi.”

10Kale nno mubeere n’amagezi mmwe bakabaka;

muyige okulabulwa mmwe abafuzi b’ensi.

112:11 a Beb 12:28 b Zab 119:119-120Muweereze Mukama nga mumutya,

era musanyuke n’okukankana.

122:12 a Yk 5:23 b Kub 6:16 c Zab 34:8; Bar 9:33Mwanirize Omwana, mumusembeze Mukama aleme okubasunguwalira

n’okubazikiriza nga muli mu kkubo lyammwe;

kubanga obusungu bwe bubuubuuka mangu.

Kyokka bonna abaddukira gy’ali balina omukisa.