Masalimo 150 – CCL & NUB

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Masalimo 150:1-6

Salimo 150

1Tamandani Yehova.

Tamandani Mulungu mʼmalo ake opatulika;

mutamandeni ku thambo lake lamphamvu.

2Mutamandeni chifukwa cha machitidwe ake amphamvu;

mutamandeni chifukwa cha ukulu wake wopambana.

3Mutamandeni poyimba malipenga,

mutamandeni ndi pangwe ndi zeze.

4Mutamandeni ndi matambolini ndi kuvina,

mutamandeni ndi zingwe ndi zitoliro.

5Mutamandeni ndi ziwaya zolira za malipenga,

mutamandeni ndi ziwaya zolira kwambiri.

6Chamoyo chilichonse chopuma chitamande Yehova.

Tamandani Yehova.

Swedish Contemporary Bible

Psaltaren 150:1-6

Psalm 150

En avslutande lovsång

1Halleluja!

Lova Gud i hans helgedom.

Lova honom i hans mäktiga himlafäste.

2Lova honom för hans väldiga gärningar.

Lova honom för hans oerhörda storhet.

3Lova honom med trumpetstötar,

med harpa och lyra.

4Lova honom med tamburiner och dans.

Lova honom med stränginstrument och flöjter.

5Lova honom med klingande cymbaler,

lova honom med ljudande cymbaler.

6Må allt som andas prisa Herren!

Halleluja!