Masalimo 15 – CCL & KLB

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Masalimo 15:1-5

Salimo 15

Salimo la Davide.

1Yehova, ndani angathe kukhala mʼmalo anu opatulika?

Kodi ndani angathe kukhala mʼphiri lanu loyera?

2Munthu wa makhalidwe abwino,

amene amachita zolungama,

woyankhula choonadi chochokera mu mtima mwake,

3ndipo mʼkamwa mwake simutuluka mawu osinjirira,

amene sachitira choyipa mnansi wake

kapena kufalitsa mbiri yoyipa ya munthu mnzake,

4amene sapereka ulemu kwa munthu woyipa.

Koma amalemekeza amene amaopa Yehova,

amene amakwaniritsa zomwe walonjeza

ngakhale pamene zikumupweteka,

5amene amakongoletsa ndalama zake popanda chiwongoladzanja

ndipo salandira chiphuphu pofuna kutsutsa anthu osalakwa.

Iye amene amachita zinthu zimenezi

sadzagwedezeka konse.

Korean Living Bible

시편 15:1-5

하나님과 교제할 수 있는 사람

(다윗의 시)

1여호와여,

누가 주의 성소에

들어갈 수 있으며

누가 주의 거룩한 산에

머물 수 있겠습니까?

2정직하게 살고

옳은 일을 행하며

그 마음에 진실을 말하는 자,

3남을 비방하지 않고

자기 친구를 해하지 않으며

이웃을 헐뜯지 않는 자,

4하나님을 저버린 자를 멸시하며

여호와를 두려워하는 자를 존중하고

한번 약속한 것은

손해가 가도 지키는 자,

5돈을 빌려 주고도

이자를 받지 않으며

뇌물을 받고

죄 없는 자를 해치지 않는 자니

이런 자들은

영원히 흔들리지 않으리라.