Masalimo 15 – CCL & BDS

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Masalimo 15:1-5

Salimo 15

Salimo la Davide.

1Yehova, ndani angathe kukhala mʼmalo anu opatulika?

Kodi ndani angathe kukhala mʼphiri lanu loyera?

2Munthu wa makhalidwe abwino,

amene amachita zolungama,

woyankhula choonadi chochokera mu mtima mwake,

3ndipo mʼkamwa mwake simutuluka mawu osinjirira,

amene sachitira choyipa mnansi wake

kapena kufalitsa mbiri yoyipa ya munthu mnzake,

4amene sapereka ulemu kwa munthu woyipa.

Koma amalemekeza amene amaopa Yehova,

amene amakwaniritsa zomwe walonjeza

ngakhale pamene zikumupweteka,

5amene amakongoletsa ndalama zake popanda chiwongoladzanja

ndipo salandira chiphuphu pofuna kutsutsa anthu osalakwa.

Iye amene amachita zinthu zimenezi

sadzagwedezeka konse.

La Bible du Semeur

Psaumes 15:1-5

Qui peut vivre avec Dieu ?

1Psaume de David.

Eternel, qui pourra séjourner ╵dans ton sanctuaire ?

Et qui donc peut demeurer ╵sur ta montagne sacrée15.1 La colline de Sion où sera bâti le temple de Jérusalem (voir 2.6). ?

2L’homme à la conduite intègre : ╵il pratique la justice,

et il dit la vérité ╵qu’il pense au fond de son cœur15.2 Autre traduction : qui, dans son cœur, cultive la vérité.,

3il ne calomnie pas son prochain,

il ne lui fait aucun mal,

et il ne s’associe pas ╵à ce qui déprécierait ses proches.

4Il méprise l’homme vil,

mais il honore celui ╵qui craint l’Eternel.

Il tient toujours ses serments ╵même s’il doit en pâtir.

5Il ne prête pas ╵de l’argent à intérêt15.5 La Loi interdisait à l’Israélite de prêter de l’argent contre intérêt à ses compatriotes (Ex 22.24 ; Dt 23.20).,

il refuse qu’on l’achète ╵pour condamner l’innocent.

Qui se conduit de la sorte ╵rien ne pourra l’ébranler.