Salimo 133
Salimo la Davide. Nyimbo yoyimba pokwera ku Yerusalemu.
1Onani, nʼkokoma ndi kokondweretsa ndithu
pamene abale akhala pamodzi mwachiyanjano!
2Zili ngati mafuta amtengowapatali othiridwa pa mutu,
otsikira ku ndevu,
ku ndevu za Aaroni,
oyenderera mpaka mʼkhosi mwa mkanjo wake.
3Zili ngati mame a ku Heremoni
otsikira pa Phiri la Ziyoni.
Pakuti pamenepo Yehova amaperekapo dalitso,
ndiwo moyo wamuyaya.
Det harmoniske fællesskab
1En valfartssang af David.
Se, hvor smukt og dejligt det er,
når Guds folk er i harmoni med hinanden.
2Det er som den kostbare salveolie,
der flyder fra Arons hoved
ned over hans skæg og præstedragt.
3Det er som den friske morgendug på Hermon,
som den livgivende regn på Zions høje.
Dér er kilden til evigt liv,
den velsignelse, Herren har lovet.