Masalimo 133 – CCL & BPH

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Masalimo 133:1-3

Salimo 133

Salimo la Davide. Nyimbo yoyimba pokwera ku Yerusalemu.

1Onani, nʼkokoma ndi kokondweretsa ndithu

pamene abale akhala pamodzi mwachiyanjano!

2Zili ngati mafuta amtengowapatali othiridwa pa mutu,

otsikira ku ndevu,

ku ndevu za Aaroni,

oyenderera mpaka mʼkhosi mwa mkanjo wake.

3Zili ngati mame a ku Heremoni

otsikira pa Phiri la Ziyoni.

Pakuti pamenepo Yehova amaperekapo dalitso,

ndiwo moyo wamuyaya.

Bibelen på hverdagsdansk

Salmernes Bog 133:1-3

Det harmoniske fællesskab

1En valfartssang af David.

Se, hvor smukt og dejligt det er,

når Guds folk er i harmoni med hinanden.

2Det er som den kostbare salveolie,

der flyder fra Arons hoved

ned over hans skæg og præstedragt.

3Det er som den friske morgendug på Hermon,

som den livgivende regn på Zions høje.

Dér er kilden til evigt liv,

den velsignelse, Herren har lovet.