Masalimo 131 – CCL & NSP

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Masalimo 131:1-3

Salimo 131

Nyimbo yoyimba pokwera ku Yerusalemu. Salimo la Davide.

1Inu Yehova, mtima wanga siwodzikuza,

maso anga siwonyada;

sinditengeteka mtima

ndi zinthu zapamwamba ndi zodabwitsa.

2Koma moyo wanga ndawutontholetsa

ndi kuwukhalitsa chete ngati mwana amene amayi ake amuletsa kuyamwa,

moyo wanga mʼkati mwanga uli ngati mwana amene amuletsa kuyamwa.

3Yembekeza Yehova, iwe Israeli,

kuyambira tsopano mpaka muyaya.

New Serbian Translation

Псалми 131:1-3

Псалам 131

Песма поклоничка. Давидова.

1О, Господе, не горди се срце моје!

Очи моје нису узносите.

Не пружам се за великим,

ни за нечим мени недосежним.

2Ево, душу сам смирио и утишао

као одојче код мајке своје,

као одојче у мени је душа моја.

3О, Израиљу, Господу се надај

од сад па довека!