Masalimo 131 – CCL & CCBT

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Masalimo 131:1-3

Salimo 131

Nyimbo yoyimba pokwera ku Yerusalemu. Salimo la Davide.

1Inu Yehova, mtima wanga siwodzikuza,

maso anga siwonyada;

sinditengeteka mtima

ndi zinthu zapamwamba ndi zodabwitsa.

2Koma moyo wanga ndawutontholetsa

ndi kuwukhalitsa chete ngati mwana amene amayi ake amuletsa kuyamwa,

moyo wanga mʼkati mwanga uli ngati mwana amene amuletsa kuyamwa.

3Yembekeza Yehova, iwe Israeli,

kuyambira tsopano mpaka muyaya.

Chinese Contemporary Bible (Traditional)

詩篇 131:1-3

第 131 篇

全心仰望上帝

大衛上聖殿朝聖之詩。

1耶和華啊,

我的心不狂傲,

我的眼目也不高傲;

我不敢涉獵太偉大、太奇妙的事。

2我的心靈平靜安穩,

如同母親身邊斷奶的孩子,

我的心靈如同斷奶的孩子。

3以色列啊,

你要仰望耶和華,

從現在直到永遠。