Masalimo 13 – CCL & NASV

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Masalimo 13:1-6

Salimo 13

Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Salimo la Davide.

1Mpaka liti Yehova? Kodi mudzandiyiwala mpaka kalekale?

Mpaka liti mudzandibisira nkhope yanu?

2Ndidzalimbana ndi maganizo anga

ndi kukhala ndi chisoni mu mtima mwanga tsiku lililonse mpaka liti?

Mpaka liti adani anga adzandipambana?

3Ndiyangʼaneni ndi kundiyankha, Inu Yehova Mulungu wanga.

Walitsani maso anga kuti ndingafe;

4mdani wanga adzati, “Ndamugonjetsa,”

ndipo adani anga adzakondwera pamene ine ndagwa.

5Koma ndikudalira chikondi chanu chosasinthika;

mtima wanga umakondwera ndi chipulumutso chanu.

6Ine ndidzayimbira Yehova

pakuti wandichitira zokoma.

New Amharic Standard Version

መዝሙር 13:1-6

መዝሙር 13

በአምላኩ የታመነ ሰው አቤቱታ

ለመዘምራን አለቃ፤ የዳዊት መዝሙር።

1እግዚአብሔር ሆይ፤ እስከ መቼ ድረስ ለዘላለሙ ትረሳኛለህ?

ፊትህንስ ከእኔ የምትሰውረው እስከ መቼ ድረስ ነው?

2ከሐሳቤ ጋር የምሟገተው፣

ልቤም ቀኑን ሙሉ የሚያዝነው እስከ መቼ ነው?

ጠላቴስ በእኔ ላይ የሚያይለው እስከ መቼ ድረስ ነው?

3እግዚአብሔር አምላኬ ሆይ፤ ተመልከት፤

ስማኝም፤

የሞት እንቅልፍ እንዳልተኛ ዐይኖቼን አብራ፤

4በዚህም ጠላቴ፣ “አሸነፍሁት” እንዳይል፣

ባላጋራዎቼም በውድቀቴ ደስ እንዳይላቸው ርዳኝ።

5እኔ ግን በጸናች ፍቅርህ እታመናለሁ፤

ልቤም በማዳንህ ደስ ይለዋል።

6ቸርነቱ በዝቶልኛልና፣

ለእግዚአብሔር እዘምራለሁ።