Masalimo 12 – CCL & AKCB

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Masalimo 12:1-8

Salimo 12

Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Monga mwa mayimbidwe seminiti. Salimo la Davide.

1Thandizeni Yehova pakuti palibe munthu wokhulupirika;

okhulupirika akusowa pakati pa anthu.

2Aliyense amanamiza mʼbale wake;

ndi pakamwa pawo pabodza amayankhula zachinyengo.

3Inu Yehova tsekani milomo yonse yachinyengo

ndi pakamwa paliponse podzikuza.

4Pakamwa pamene pamati, “Ife tidzapambana ndi kuyankhula kwathu;

pakamwapa ndi pathupathu, tsono mbuye wathu ndani?”

5“Chifukwa cha kuponderezedwa kwa anthu opanda mphamvu

ndi kubuwula kwa anthu osowa,

Ine ndidzauka tsopano,” akutero Yehova,

“Ndidzawateteza kwa owazunza.”

6Ndipo mawu a Yehova ndi angwiro

monga siliva oyengedwa mʼngʼanjo yadothi,

oyengedwa kasanu nʼkawiri.

7Inu Yehova mudzatitchinjiriza ndipo

mudzatiteteza kwa anthu otere kwamuyaya.

8Oyipa amangoyendayenda ponseponse

anthu akamayamikira zochita zawo.

Akuapem Twi Contemporary Bible

Nnwom 12:1-8

Dwom 12

Dawid dwom.

1Boa yɛn, Awurade, na nyamesurofo asa;

nokwafo ayera wɔ nnipa mu.

2Obiara di atoro kyerɛ ne yɔnko;

wɔn ano a ɛdɛfɛdɛfɛ no ka nnaadaasɛm.

3Ma Awurade ntwa nnaadaa ano

ne tɛkrɛma biara a ɛhoahoa ne ho nkyene;

4nea ɛka se, “Yɛde yɛn tɛkrɛma bedi nkonim;

yɛn ano bedi ama yɛn, na hena na odi yɛn so tumi?”

5“Esiane ɔhyɛ a wɔde hyɛ mmɔborɔni

ne ohiani apinisi no nti,

mɛsɔre afei,” Awurade na ose.

“Mɛbɔ wɔn ho ban afi wɔn a wɔhaw wɔn no ho.”

6Awurade asɛm yɛ nokware

te sɛ dwetɛ a wɔasɔn so wɔ fononoo mu,

na wɔahoa ho mpɛn ason.

7Awurade, wobɛkora mmɔborɔni

na woabɔ yɛn ho ban afi saa nnipa yi ho afebɔɔ.

8Amumɔyɛfo nenam sɛnea wɔpɛ,

bere a adesamma de nidi ma afide.