Masalimo 114 – CCL & TNCV

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Masalimo 114:1-8

Salimo 114

1Pamene Israeli anatuluka mu Igupto,

nyumba ya Yakobo kuchoka ku mtundu wa anthu a chiyankhulo chachilendo,

2Yuda anasanduka malo opatulika a Mulungu,

Israeli anasanduka ufumu wake.

3Nyanja inaona ndi kuthawa,

mtsinje wa Yorodani unabwerera mʼmbuyo;

4mapiri analumphalumpha ngati nkhosa zazimuna,

timapiri ngati ana ankhosa.

5Nʼchifukwa chiyani iwe unathawa?

iwe mtsinje wa Yorodani unabwereranji mʼmbuyo?

6inu mapiri, munalumphalumphiranji ngati nkhosa zazimuna,

inu timapiri, ngati ana ankhosa?

7Njenjemera pamaso pa Ambuye iwe dziko lapansi,

pamaso pa Mulungu wa Yakobo,

8amene anasandutsa thanthwe kukhala chitsime,

thanthwe lolimba kukhala akasupe a madzi.

Thai New Contemporary Bible

สดุดี 114:1-8

สดุดี 114

1เมื่ออิสราเอลออกจากอียิปต์

วงศ์วานของยาโคบออกจากชนต่างภาษา

2ยูดาห์กลายเป็นสถานนมัสการของพระเจ้า

อิสราเอลเป็นอาณาจักรของพระองค์

3ทะเลมองดูแล้วถอยหนี

แม่น้ำจอร์แดนหันกลับ

4ภูเขาทั้งหลายโลดเต้นเหมือนแกะผู้

เนินเขากระโดดเหมือนลูกแกะ

5ทะเลเอ๋ย เหตุใดเจ้าจึงถอยหนี?

แม่น้ำจอร์แดนเอ๋ย เหตุใดเจ้าจึงหันกลับ?

6ภูเขาเอ๋ย เหตุใดจึงโลดเต้นเหมือนแกะผู้?

เนินเขาเอ๋ย เหตุใดจึงกระโดดเหมือนลูกแกะ?

7แผ่นดินโลกเอ๋ย จงสั่นสะท้านต่อหน้าองค์พระผู้เป็นเจ้า

ต่อหน้าพระเจ้าของยาโคบ

8ผู้ทรงทำให้หินกลายเป็นแอ่งน้ำ

ศิลาแกร่งกลายเป็นธารน้ำพุ