Salimo 111
1Tamandani Yehova.
Ndidzathokoza Yehova ndi mtima wanga wonse
mʼbwalo la anthu olungama mtima ndi pa msonkhano.
2Ntchito za Yehova nʼzazikulu;
onse amene amakondwera nazo amazilingalira.
3Zochita zake ndi za ulemerero ndi zaufumu,
ndipo chilungamo chake ndi chosatha.
4Iye wachititsa kuti zodabwitsa zake zikumbukirike;
Yehova ndi wokoma mtima ndi wachifundo.
5Amapereka chakudya kwa amene amamuopa Iye;
amakumbukira pangano lake kwamuyaya.
6Waonetsa anthu ake mphamvu ya ntchito zake,
kuwapatsa mayiko a anthu a mitundu ina.
7Ntchito za manja ake ndi zokhulupirika ndi zolungama;
malangizo ake onse ndi odalirika.
8Malamulo ndi okhazikika ku nthawi za nthawi,
ochitidwa mokhulupirika ndi molungama.
9Iyeyo amawombola anthu ake;
anakhazikitsa pangano lake kwamuyaya
dzina lake ndi loyera ndi loopsa.
10Kuopa Yehova ndicho chiyambi cha nzeru;
onse amene amatsatira malangizo ake amamvetsa bwino zinthu.
Iye ndi wotamandika mpaka muyaya.
Песнь 111Песнь 111 В оригинале эта песнь написана в форме акростиха: каждая строка начинается с очередной буквы еврейского алфавита.
Славьте Вечного!
1Благословен человек, боящийся Вечного,
кому в радость исполнять Его повеления.
2Могущественным будет на земле его потомство;
поколение праведных благословится.
3Изобилие и богатство будут в его доме,
и воздаяние за его праведность пребудет вовек.
4Для честных даже во тьме восходит свет,
для тех, кто милостив, милосерден и праведен111:4 Или: «…восходит свет, потому что Всевышний милостив, милосерден и праведен»..
5Благо человеку, который великодушен и щедро даёт взаймы,
тому, кто ведёт свои дела справедливо.
6Он никогда не поколеблется;
праведник никогда не будет забыт.
7Не побоится плохих известий;
сердце его твёрдо – он надеется на Вечного.
8Сердце его крепко – он не испугается;
он увидит падение своих врагов.
9Он щедро раздал своё имущество бедным,
и его праведность пребудет вовек;
он будет силён и прославлен111:9 Букв.: «его рог вознесётся в славе». Рог был символом могущества, власти и силы..
10Нечестивый увидит и разозлится,
заскрипит зубами и исчезнет.
Желание нечестивых не сбудется.