Masalimo 11 – CCL & NSP

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Masalimo 11:1-7

Salimo 11

Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Salimo la Davide.

1Mwa Yehova ine ndimathawiramo.

Nanga mungathe bwanji kunena kwa ine kuti,

“Thawira ku phiri lako ngati mbalame.

2Pakuti taona oyipa akunga mauta awo;

ayika bwino mivi yawo pa zingwe za uta,

pobisala pawo kuti alase

olungama mtima.

3Tsono ngati maziko awonongeka,

olungama angachite chiyani?”

4Yehova ali mʼNyumba yake yoyera;

Yehova ali pa mpando wake waufumu kumwamba.

Iye amayangʼanitsitsa ana a anthu;

maso ake amawayesa.

5Yehova amayesa olungama,

koma moyo wake umadana ndi oyipa,

amene amakonda zachiwawa.

6Iye adzakhuthulira pa oyipa

makala amoto ndi sulufule woyaka;

mphepo yotentha idzakhala yowayenera.

7Pakuti Yehova ndi wolungama,

Iye amakonda chilungamo;

ndipo anthu olungama adzaona nkhope yake.

New Serbian Translation

Псалми 11:1-7

Псалам 11

Хоровођи. Давидов.

1Уточиште је мени у Господу.

Зашто онда мени говорите:

„Као птица у гору утеци!

2Јер, гле, опаки лук свој натежу,

на тетиву стрелу постављају,

да поштене из мрака гађају.

3Када се темељи распадају,

шта праведник може да учини?“

4Господ је у свом светом храму,

Господњи је престо на небесима,

очима он помно посматра,

он прониче потомке људи.

5Праведнога испитује Господ,

али душа његова мрзи онога,

ко је опак и воли насиље.

6На опаког он ће сручити

ужарено угљевље и сумпор;

пламенови огњеног вихора,

то је део њихов, то им је у чаши.

7Јер праведан је Господ,

праведност он воли,

поштени ће гледати му лице.