Hoseya 4 – CCL & LCB

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Hoseya 4:1-19

Yehova Ayimba Mlandu Israeli

1Inu Aisraeli, imvani mawu a Yehova,

chifukwa Yehova ali ndi mlandu ndi inu

amene mumakhala mʼdzikoli:

“Mʼdziko mwanu mulibe kukhulupirika, mulibe chikondi

mulibe kulabadira za Mulungu.

2Muli kutemberera kokha, kunama ndi kupha.

Kuba ndi kuchita chigololo;

machimo achita kunyanya

ndipo akungokhalira kuphana.

3Chifukwa chake dziko likulira

ndipo onse amene amakhalamo akuvutika;

zirombo zakuthengo ndi mbalame zamumlengalenga

ndiponso nsomba zamʼnyanja zikufa.

4“Koma wina asapeze mnzake chifukwa,

wina aliyense asayimbe mlandu mnzake,

pakuti anthu ako ali ngati anthu

amene amayimba mlandu wansembe.

5Mumapunthwa usana ndi usiku

ndipo aneneri amapunthwa nanu pamodzi.

Choncho ndidzawononga amayi anu.

6Anthu anga akuwonongeka chifukwa chosadziwa.

“Pakuti mwakana kudziwa,

Inenso ndidzakukanani monga ansembe anga;

chifukwa mwayiwala lamulo la Mulungu wanu,

Inenso ndidzayiwala ana anu.

7Ansembe ankati akachuluka

iwo ankandichimwiranso kwambiri;

iwo anasinthanitsa ulemerero wawo ndi chinthu china chonyansa.

8Amalemererapo pa machimo a anthu anga

ndipo amafunitsitsa kuti anthuwo azipitiriza kuchimwa.

9Ndipo zidzakhala motere: zochitikira anthu ena, zidzachitikiranso ansembe.

Ndidzawalanga onsewo chifukwa cha njira zawo,

ndidzawabwezera chifukwa cha machitidwe awo.

10“Iwo azidzadya koma sadzakhuta;

azidzachita zachiwerewere koma sadzachulukana,

chifukwa anasiya Yehova

kuti adzipereke 11ku zachiwerewere,

ku vinyo wakale ndi watsopano,

zimene zimachotsa nzeru zomvetsa zinthu

12za anthu anga.

Anthu anga amapempha nzeru ku fano lamtengo

ndipo ndodo yawo yamtengo imawayankha.

Mzimu wachiwerewere umawasocheretsa;

iwo sakukhulupirika kwa Mulungu wawo.

13Amapereka nsembe pamwamba pa mapiri

ndi kufukiza lubani pa zitunda,

pa tsinde pa mtengo wa thundu, mnjale ndi mkundi,

pamene pali mthunzi wabwino.

Nʼchifukwa chake ana anu aakazi akuchita zachiwerewere

ndipo akazi a ana anu akuchita zigololo.

14“Ine sindidzalanga ana anu aakazi

pamene iwo adzachita zachiwerewere,

kapena akazi a ana anu

pamene adzachita zigololo.

Paja inu nomwe amunanu mumayenda ndi akazi achiwerewere,

ndipo mumapereka nsembe pamodzi ndi akazi achiwerewere a ku malo opembedzerako.

Anthu amene alibe nzeru adzawonongeka ndithu!

15“Ngakhale umachita chigololo, iwe Israeli,

Yuda asapezeke ndi mlandu wotere.

“Usapite ku Giligala.

Usapite ku Beti-Aveni.

Ndipo usalumbire kuti, ‘Pali Yehova wamoyo!’

16Aisraeli ndi nkhutukumve,

ngosamva ngati ana angʼombe.

Kodi Yehova angathe kuwaweta bwanji

ngati ana ankhosa pa msipu wabwino?

17Efereimu waphathana ndi mafano;

mulekeni!

18Ngakhale pamene zakumwa zawo zatha,

amapitiriza kuchita zachiwerewere;

atsogoleri awo amakonda kwambiri njira zawo zochititsa manyazi.

19Adzachotsedwa ndi kamvuluvulu

ndipo adzachita manyazi chifukwa cha nsembe zawo.

Luganda Contemporary Bible

Koseya 4:1-19

Okulabula eri Isirayiri

14:1 Yer 7:28Muwulire ekigambo kya Mukama, mmwe abantu ba Isirayiri,

kubanga Mukama abalinako ensonga

mmwe abatuula mu nsi.

“Obwesigwa n’okwagala Katonda,

n’okumumanya bikendedde mu nsi.

24:2 a Kos 7:3; 10:4 b Kos 6:9 c Kos 7:1Waliwo okukolima, n’okulimba, n’okutta,

n’okubba, n’okukola eby’obwenzi;

bawaguza,

era bayiwa omusaayi obutakoma.

34:3 a Yer 4:28 b Is 33:9 c Yer 4:25; Zef 1:3Ensi kyeneeva ekaaba,

ne bonna abagibeeramu ne bafuuka ekitagasa;

n’ensolo enkambwe ez’omu nsiko zirifa, n’ennyonyi ez’omu bbanga nazo zirifa,

n’ebyennyanja ebiri mu nnyanja ne bifa.

44:4 Ma 17:12; Ez 3:26“Naye temuloopagana,

so tewabaawo muntu avunaana munne,

kubanga ensonga

ngivunaana gwe kabona.

54:5 a Ez 14:7 b Kos 2:2Wakola ebibi emisana n’ekiro,

ne bannabbi ne babikolera wamu naawe;

kyendiva nzikiriza maama4:5 maama kitegeeza Obwakabaka bwa Isirayiri wo.

64:6 a Kos 2:13; Mal 2:7-8 b Kos 8:1, 12Abantu bange bazikiridde olw’obutamanya.

“Kyemunaava mulema

okubeera bakabona bange;

era olw’okulagajjalira etteeka lya Katonda wo,

nange kyendiva ndagajjalira abaana bo.

74:7 a Kbk 2:16 b Kos 10:1, 6; 13:6Gye beeyongera okuba abangi,

gye baakoma n’okukola ebibi;

baasuula ekitiibwa kyabwe ne banswaza.

84:8 Is 56:11; Mi 3:11Bagaggawalira ku bibi by’abantu bange,

era basemba okwonoona kwabwe.

94:9 a Is 24:2 b Yer 5:31; Kos 8:13; 9:9, 15Era bwe kityo bwe kiriba eri abantu n’eri bakabona:

ndibabonereza olw’enneeyisa yaabwe,

era ne mbasasula ng’ebikolwa byabwe.

104:10 a Lv 26:26; Mi 6:14 b Kos 7:14; 9:17“Balirya naye tebalikkuta,

balikola ebibi eby’obwenzi kyokka tebalyeyongera bungi,

kubanga bavudde ku Mukama ne beewaayo 114:11 a Kos 5:4 b Nge 20:1eri obwenzi,

wayini omukadde n’omusu,

ne bibamalamu okutegeera. 124:12 a Yer 2:27 b Kbk 2:19 c Is 44:20Abantu bange

beebuuza ku kikonge ky’omuti,

ne baddibwamu omuti.

Omwoyo ogw’obwenzi gubasendasenda

ne gubaleetera obutaba beesigwa eri Katonda waabwe.

134:13 a Is 1:29 b Yer 3:6; Kos 11:2 c Yer 2:20; Am 7:17 d Kos 2:13Baweerayo ssaddaaka ku ntikko z’ensozi,

ne baweerayo ebiweebwayo ebyokebwa ku busozi,

wansi w’emyalooni, n’emiribine n’emyera

awali ekisiikirize ekirungi.

Bawala bammwe kyebava baba bamalaaya,

ne baka baana bammwe ne bakola obwenzi.

144:14 nny 11“Siribonereza bawala bammwe

olw’okubeera bamalaaya,

newaakubadde baka baana bammwe

okukola eby’obwenzi,

kubanga abasajja bennyini bassa bumu ne bamalaaya,

ne baweerayo ssaddaaka ne bamalaaya ab’omu masabo;

abantu abatategeera balizikirira.

154:15 Kos 9:15; 12:11; Am 4:4“Newaakubadde ggwe Isirayiri oyenda,

omusango guleme okuba ku Yuda.

Togenda Girugaali,

newaakubadde okwambuka e Besaveni.4:15 Besaveni kitegeeza ennyumba ey’abakozi b’ebibi

Tolayiranga nti, ‘Nga Katonda bw’ali omulamu.’

164:16 Is 5:17; 7:25Abayisirayiri bakakanyavu mu mitima

ng’ennyana endalu.

Olwo Mukama ayinza atya okubalabirira

ng’abaana b’endiga abali mu kisibo?

17Efulayimu yeegasse n’abasinza ebifaananyi,

mumuleke abeere yekka.

18Ebyokunywa ne bwe bibaggwaako,

beeyongera mu bwamalaaya;

n’abakulembeze baabwe baagala nnyo eby’ensonyi:

194:19 a Kos 12:1; 13:15 b Is 1:29Embuyaga kyeziriva zibatwala,

ne ssaddaaka zaabwe ne zibaswaza.”