Kumvera Aulamuliro
1Aliyense ayenera kumvera akulu olamulira, chifukwa palibe ulamuliro umene sunachokere kwa Mulungu. Olamulira amene alipo anayikidwa ndi Mulungu. 2Kotero kuti, iwo amene awukira ulamuliro atsutsana ndi chimene Mulungu anakhazikitsa. Ndipo amene atero adzibweretsera okha chilango. 3Pakuti olamulira saopseza amene amachita zabwino koma amene amachita zoyipa. Kodi mukufuna kukhala osaopa olamulira? Tsono chitani zoyenera ndipo adzakuyamikirani. 4Pakuti iyeyo ndi mtumiki wa Mulungu wokuchitirani zabwino. Koma ngati muchita zoyipa muchite mantha, pakuti iye ali ndi mphamvu zolangira. Iye ndi mtumiki wa Mulungu wobweretsa mkwiyo ndi kulanga onse ochita zoyipa. 5Nʼchifukwa chake ndi koyenera kugonjera olamulira, osati chifukwa choopa kulangidwa kokha komanso chifukwa cha chikumbumtima. 6Ichi nʼchifukwa chakenso inu mumapereka msonkho. Pakuti olamulira ndi atumiki a Mulungu amene amapereka nthawi yawo yonse kulamulira. 7Mubwezereni aliyense amene munamukongola. Ngati inu muli ndi ngongole yamsonkho, perekani msonkho kwa oyenera kuwalipira. Ngati ndi kuopa perekeni kwa oyenera kuwaopa ndipo ngati ndi ulemu kwa oyenera ulemu.
Chikondi Chimakwaniritsa Malamulo
8Musakhale ndi ngongole ndi wina aliyense kupatula ngongole ya kukondana wina ndi mnzake. Pakuti amene amakonda munthu mnzake wakwaniritsa lamulo. 9Malamulo awa: “Usachite chigololo,” “Usaphe,” “Usabe,” “Usasirire,” ndi malamulo ena onse amene alipo, akhazikika pa lamulo limodzi ili, “Konda mnansi wako monga iwe mwini.” 10Chikondi sichichitira mnzake zoyipa. Chifukwa chake chikondi ndicho chokwaniritsa lamulo.
11Ndipo chitani ichi pozindikira nthawi ino. Nthawi yafika yoti inu mudzuke kutulo, chifukwa chipulumutso chathu chili pafupi tsopano kuposa pamene tinayamba kukhulupirira. 12Usiku watsala pafupifupi kutha. Kwatsala pangʼono kucha. Tiyeni tsono tichotse ntchito zamdima ndipo tivale chovala chakuwunika. 13Tiyeni tikhale moyenera monga nthawi ya masana, osati mʼmagulu amadyerero, achiwerewere ndi kuledzera, mʼmadama ndi zonyansa komanso osati mʼmagawano ndi nsanje. 14Koma valani Ambuye Yesu Khristu ndipo musaganizire za momwe mungakwaniritsire zokhumba zachikhalidwe cha uchimo.
وظيفهٔ مسيحيان نسبت به دولت
1مطيع دولت و قوانين آن باشيد، زيرا آن را خدا برقرار كرده است. در تمام نقاط جهان، همهٔ دولتها را خدا بر سر قدرت آورده است. 2پس هر كه از قوانين كشور سرپيچی كند، در واقع از خدا نااطاعتی كرده است، و البته مجازات خواهد شد. 3آنانی كه اعمالشان درست است، از مأموران دولت هراسی ندارند، اما افراد خطاكار و نادرست هميشه از آنان میترسند. پس اگر میخواهی در ترس و دلهره به سر نبری، قوانين را اطاعت كن و آسوده باش! 4مأمور دولت از جانب خدا وظيفه دارد به تو كمک كند. اما اگر كار خلافی انجام دهی، از او بترس زيرا تو را مجازات خواهد كرد. خدا او را مقرر كرده تا كسانی را كه خلاف میكنند مجازات كند. 5پس به دو دليل بايد مطيع قانون باشی: اول برای اينكه مجازات نشوی؛ و دوم برای اينكه میدانی اطاعت، وظيفهٔ توست.
6به همين دو دليل نيز بايد مالياتهايتان را بپردازيد تا حقوق كاركنان دولت تأمين شود و بتوانند به انجام كار خدا، يعنی خدمت به شما ادامه دهند. 7حق هر كس را به او ادا كنيد: مالياتها را از روی ميل بپردازيد؛ از افراد مافوق خود اطاعت نماييد؛ و به آنانی كه سزاوار احترامند، احترام كنيد.
وظيفهٔ مسيحيان نسبت به مردم
8تمام بدهیهای خود را بپردازيد تا به كسی مديون نباشيد. فقط خود را مديون بدانيد كه مردم را محبت كنيد. هرگز از محبت نمودن باز نايستيد زيرا با محبت كردن به ديگران، در واقع از احكام الهی اطاعت كردهايد و خواست خدا را بجا آوردهايد. 9اگر همسايه و همنوع خود را به همان اندازه دوست بداريد كه خود را دوست میداريد، هرگز راضی نخواهيد شد كه به او صدمه بزنيد، يا فريبش دهيد، يا او را به قتل برسانيد و يا مالش را بدزديد؛ و هرگز به زن و به اموال او چشم طمع نخواهيد دوخت؛ خلاصه، هيچيک از كارهايی را كه خدا در ده فرمان منع كرده است، انجام نخواهيد داد. بنابراين، ده فرمان در اين فرمان خلاصه میشود كه «همسايهٔ خود را دوست بدار، به همان اندازه كه خود را دوست میداری.» 10بلی، محبت به هيچكس بدی نمیكند. پس اگر به انسانها محبت نماييد، مانند آنست كه همهٔ دستورات و احكام الهی را بجا آوردهايد. خلاصه، تنها حكم و قانونی كه لازم داريد، محبت است.
11مسئلهٔ ديگری كه ما را به انجام اعمال نيک ترغيب میكند، اينست كه وقت به سرعت میگذرد و عمر ما به پايان میرسد. پس بيدار شويد زيرا اكنون وقت بازگشت خداوند نزديكتر است از آن زمانی كه ايمان آورديم. 12-13«شب» به پايان خود رسيده و «روز» نزديک است. بنابراين، اعمال گناهآلود تاريكی را كنار گذارده، در نور خدا زندگی پاک و مقدسی را در پيش گيريد، زيرا اين وظيفهٔ ماست كه در نور زندگی كنيم! آنچه میكنيد با شايستگی باشد. از حضور در محافل عياشی و نيز از مستی و زنا و شهوترانی و دعوا و حسادت بپرهيزيد. 14تمام وجودتان از آن مسيح باشد؛ به دنبال هوسهای جسم نرويد.