1 Mbiri 1 – CCL & KJV

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

1 Mbiri 1:1-54

Mbiri ya Makolo Kuchokera pa Adamu Mpaka pa Abrahamu

Mpaka pa Ana a Nowa

1Adamu, Seti, Enosi 2Kenani, Mahalaleli, Yaredi, 3Enoki, Metusela, Lameki, Nowa.

4Ana a Nowa,

Semu, Hamu ndi Yafeti.

Fuko la Yafeti

5Ana aamuna a Yafeti anali:

Gomeri, Magogi, Madai, Yavani, Tubala, Mesaki ndi Tirasi.

6Ana aamuna a Gomeri anali:

Asikenazi, Rifati ndi Togarima

7Ana aamuna a Yavani anali:

Elisa, Tarisisi, Kitimu ndi Rodanimu.

Fuko la Hamu

8Ana aamuna a Hamu anali:

Kusi, Miziraimu, Puti ndi Kanaani

9Ana aamuna a Kusi anali:

Seba, Havila, Sabita, Raama ndi Sabiteka

Ana aamuna a Raama anali:

Seba ndi Dedani.

10Kusi anali abambo a Nimurodi amene anali wankhondo wamphamvu

kwambiri pa dziko lapansi.

11Igupto ndiye kholo la

Aludi, Aanami, Alehabu, Anafutu, 12Apaturusi, Akasilu (kumene kunachokera Afilisti) ndi Akafitori.

13Kanaani anabereka mwana wake wachisamba Sidoni,

ndipo anaberekanso Ahiti, 14Ayebusi, Aamori, Agirigasi 15Ahivi, Aariki, Asini 16Aaravadi, Azemari ndi Ahamati.

Fuko la Semu

17Ana aamuna a Semu anali:

Elamu, Asuri, Aripakisadi, Ludi ndi Aramu.

Ana aamuna a Aramu anali:

Uzi, Huri, Geteri ndi Mesaki.

18Aripakisadi anabereka Sela

ndipo Selayo anabereka Eberi:

19Eberi anabereka ana aamuna awiri:

wina anamutcha Pelegi, chifukwa pa nthawiyo anthu a pa dziko lapansi anagawikana. Dzina la mʼbale wake linali Yokitani.

20Yokitani anabereka

Alimodadi, Selefi, Hazari-Maveti, Yera, 21Hadoramu, Uzali, Dikila 22Obali, Abimaeli, Seba, 23Ofiri, Havila ndi Yobabu. Onsewa anali ana aamuna a Yokitani.

24Semu, Aripakisadi, Sela

25Eberi, Pelegi, Reu

26Serugi, Nahori, Tera

27ndi Abramu (amene ndi Abrahamu).

Banja la Abrahamu

28Ana a Abrahamu ndi awa:

Isake ndi Ismaeli.

Zidzukulu za Hagara

29Zidzukulu zake zinali izi:

Nebayoti ndiye anali mwana woyamba wa Ismaeli, kenaka Kedara, Adibeeli, Mibisamu, 30Misima, Duma, Masa, Hadadi, Tema, 31Yeturi, Nafisi ndi Kedema. Awa anali ana a Ismaeli.

Zidzukulu za Ketura

32Ana a Ketura mzikazi wa Abrahamu anali awa:

Zimurani, Yokisani, Medani, Midiyani, Isibaki ndi Suwa.

Ana a Yokisani ndi awa:

Seba ndi Dedani

33Ana aamuna a Midiyani anali,

Efai, Eferi, Hanoki, Abida ndi Elida.

Onsewa anali zidzukulu za Ketura.

Zidzukulu za Sara

34Abrahamu anabereka Isake.

Ana a Isake anali awa:

Esau ndi Israeli.

Ana a Esau

35Ana aamuna a Esau anali awa:

Elifazi, Reueli, Yeusi, Yolamu ndi Kora.

36Ana a Elifazi anali awa:

Temani, Omari, Zefo, Gatamu ndi Kenazi:

Amene anabereka ndi Timna: Amaleki.

37Ana a Reueli anali awa:

Nahati, Zera, Sama ndi Miza.

Anthu a ku Seiri ku Edomu

38Ana a Seiri anali awa:

Lotani, Sobala, Zibeoni, Ana, Disoni, Ezeri ndi Disani.

39Ana aamuna a Lotani anali awa:

Hori ndi Homamu. Timna anali mlongo wake wa Lotani.

40Ana aamuna a Sobala anali awa:

Alivani, Manahati, Ebala, Sefo ndi Onamu.

Ana aamuna a Zibeoni anali awa:

Ayiwa ndi Ana.

41Mwana wa Ana anali

Disoni.

Ana a Disoni anali awa:

Hemudani, Esibani, Itirani ndi Kerani

42Ana aamuna a Ezeri anali awa:

Bilihani, Zaavani ndi Yaakani.

Ana aamuna a Disani anali awa:

Uzi ndi Arani.

Mafumu a ku Edomu

43Awa ndi mafumu amene ankalamulira dziko la Edomu, mfumu iliyonse ya Israeli isanayambe kulamulira kumeneko:

Bela mwana wa Beori, mzinda wake ankawutcha Dinihaba.

44Bela atamwalira, Yobabu mwana wa Zera wochokera ku Bozira analowa ufumu mʼmalo mwake.

45Yobabu atamwalira, Husamu wochokera ku dziko la Atemani, analowa ufumu mʼmalo mwake.

46Husamu atamwalira, Hadadi mwana wa Bedadi, amene anagonjetsa Amidiyani mʼdziko la Mowabu, analowa ufumu mʼmalo mwake. Mzinda wake unkatchedwa Aviti.

47Hadadi atamwalira, Samila wochokera ku Masireka analowa ufumu mʼmalo mwake.

48Samila atamwalira, Sauli wochokera ku Rehoboti wa ku Mtsinje analowa ufumu mʼmalo mwake.

49Sauli atamwalira, Baala-Hanani mwana wa Akibori analowa ufumu mʼmalo mwake.

50Pamene Baala-Hanani anamwalira, Hadadi analowa ufumu mʼmalo mwake. Mzinda wake unkatchedwa Pau, ndipo dzina la mkazi wake linali Mehatabeli mwana wa Matiredi, mwana wamkazi wa Me-Zahabu. 51Hadadi anamwaliranso.

Mafumu a ku Edomu anali:

Timna, Aliva, Yeteti, 52Oholibama, Ela, Pinoni, 53Kenazi, Temani, Mibezari, 54Magidieli ndi Iramu. Awa anali mafumu a ku Edomu.

King James Version

1 Chronicles 1:1-54

1Adam, Sheth, Enosh, 2Kenan, Mahalaleel, Jered, 3Henoch, Methuselah, Lamech, 4Noah, Shem, Ham, and Japheth.

5¶ The sons of Japheth; Gomer, and Magog, and Madai, and Javan, and Tubal, and Meshech, and Tiras. 6And the sons of Gomer; Ashchenaz, and Riphath, and Togarmah.1.6 Riphath: or, Diphath as it is in some copies 7And the sons of Javan; Elishah, and Tarshish, Kittim, and Dodanim.1.7 Dodanim: or, Rodanim, according to some copies

8¶ The sons of Ham; Cush, and Mizraim, Put, and Canaan. 9And the sons of Cush; Seba, and Havilah, and Sabta, and Raamah, and Sabtecha. And the sons of Raamah; Sheba, and Dedan. 10And Cush begat Nimrod: he began to be mighty upon the earth. 11And Mizraim begat Ludim, and Anamim, and Lehabim, and Naphtuhim, 12And Pathrusim, and Casluhim, (of whom came the Philistines,) and Caphthorim. 13And Canaan begat Zidon his firstborn, and Heth, 14The Jebusite also, and the Amorite, and the Girgashite, 15And the Hivite, and the Arkite, and the Sinite, 16And the Arvadite, and the Zemarite, and the Hamathite.

17¶ The sons of Shem; Elam, and Asshur, and Arphaxad, and Lud, and Aram, and Uz, and Hul, and Gether, and Meshech.1.17 Meshech: or, Mash 18And Arphaxad begat Shelah, and Shelah begat Eber. 19And unto Eber were born two sons: the name of the one was Peleg; because in his days the earth was divided: and his brother’s name was Joktan.1.19 Peleg: that is, division 20And Joktan begat Almodad, and Sheleph, and Hazarmaveth, and Jerah, 21Hadoram also, and Uzal, and Diklah, 22And Ebal, and Abimael, and Sheba, 23And Ophir, and Havilah, and Jobab. All these were the sons of Joktan.

24¶ Shem, Arphaxad, Shelah, 25Eber, Peleg, Reu, 26Serug, Nahor, Terah, 27Abram; the same is Abraham.

28The sons of Abraham; Isaac, and Ishmael.

29¶ These are their generations: The firstborn of Ishmael, Nebaioth; then Kedar, and Adbeel, and Mibsam, 30Mishma, and Dumah, Massa, Hadad, and Tema,1.30 Hadad: also called, Hadar 31Jetur, Naphish, and Kedemah. These are the sons of Ishmael.

32¶ Now the sons of Keturah, Abraham’s concubine: she bare Zimran, and Jokshan, and Medan, and Midian, and Ishbak, and Shuah. And the sons of Jokshan; Sheba, and Dedan. 33And the sons of Midian; Ephah, and Epher, and Henoch, and Abida, and Eldaah. All these are the sons of Keturah. 34And Abraham begat Isaac. The sons of Isaac; Esau and Israel.

35¶ The sons of Esau; Eliphaz, Reuel, and Jeush, and Jaalam, and Korah. 36The sons of Eliphaz; Teman, and Omar, Zephi, and Gatam, Kenaz, and Timna, and Amalek.1.36 Zephi: or, Zepho 37The sons of Reuel; Nahath, Zerah, Shammah, and Mizzah. 38And the sons of Seir; Lotan, and Shobal, and Zibeon, and Anah, and Dishon, and Ezer, and Dishan. 39And the sons of Lotan; Hori, and Homam: and Timna was Lotan’s sister.1.39 Homam: or, Hemam 40The sons of Shobal; Alian, and Manahath, and Ebal, Shephi, and Onam. And the sons of Zibeon; Aiah, and Anah.1.40 Alian: also called, Alvan1.40 Shephi: also called, Shepho 41The sons of Anah; Dishon. And the sons of Dishon; Amram, and Eshban, and Ithran, and Cheran.1.41 Amram: or, Hemdan 42The sons of Ezer; Bilhan, and Zavan, and Jakan. The sons of Dishan; Uz, and Aran.1.42 Jakan: or, Akan

43¶ Now these are the kings that reigned in the land of Edom before any king reigned over the children of Israel; Bela the son of Beor: and the name of his city was Dinhabah. 44And when Bela was dead, Jobab the son of Zerah of Bozrah reigned in his stead. 45And when Jobab was dead, Husham of the land of the Temanites reigned in his stead. 46And when Husham was dead, Hadad the son of Bedad, which smote Midian in the field of Moab, reigned in his stead: and the name of his city was Avith. 47And when Hadad was dead, Samlah of Masrekah reigned in his stead. 48And when Samlah was dead, Shaul of Rehoboth by the river reigned in his stead. 49And when Shaul was dead, Baal-hanan the son of Achbor reigned in his stead. 50And when Baal-hanan was dead, Hadad reigned in his stead: and the name of his city was Pai; and his wife’s name was Mehetabel, the daughter of Matred, the daughter of Mezahab.1.50 Hadad: or, Hadar1.50 Pai: or, Pau

51¶ Hadad died also. And the dukes of Edom were; duke Timnah, duke Aliah, duke Jetheth, 52Duke Aholibamah, duke Elah, duke Pinon, 53Duke Kenaz, duke Teman, duke Mibzar, 54Duke Magdiel, duke Iram. These are the dukes of Edom.