約翰一書 1 – CCBT & CCL

Chinese Contemporary Bible (Traditional)

約翰一書 1:1-10

生命之道

1論到從太初就已經存在的生命之道,我們曾經耳聞目睹,親眼看過,親手摸過。 2這生命曾顯現過,我們看見了,現在做見證,向你們傳揚這原本與父同在、曾向我們顯現的永恆生命。 3我們把所見所聞傳給你們,使你們可以與我們相交。誠然,我們是與父和祂兒子耶穌基督相交。 4我們將這些話寫給你們,是要讓大家都充滿喜樂。

要活在光中

5我們從耶穌那裡聽見、現在傳給你們的信息就是:上帝是光,在祂裡面毫無黑暗。 6如果我們說與祂相交,卻仍過著黑暗的生活,就是撒謊,沒有遵行真理。 7如果我們生活在光明之中,像上帝在光明中一樣,就能夠彼此相交,上帝兒子耶穌的血能洗淨我們一切的罪。

8如果我們說自己沒有罪,便是自欺,真理就不在我們心中。 9如果我們承認自己的罪,上帝是信實公義的,必赦免我們的罪,洗淨我們一切的不義。 10我們如果說自己沒有犯過罪,就是把上帝看作說謊的,祂的道也不在我們心中。

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

1 Yohane 1:1-10

Mawu a Moyo

1Tikukulalikirani za Mawu a moyo amene analipo kuyambira pachiyambi, amene tinawamva, amene tinawaona ndi maso athu, amene tinawapenyetsetsa, ndipo tinawakhudza ndi manja athu. 2Moyowo unaoneka, tinawuona ndipo tikuchitira umboni. Tikukulalikirani za moyo wosatha umene unali ndi Atate ndipo unaonekera kwa ife. 3Tikukulalikirani chimene tinachiona ndi kumva, kuti inuyo muyanjane nafe. Kuyanjana kwathu, tikuyanjana ndi Atate ndiponso ndi Mwana wawo, Yesu Khristu. 4Tikukulemberani zimenezi kuti chimwemwe chathu chikhale chathunthu.

Kuyenda mu Kuwunika

5Uthenga umene tinamva kwa Iye ndipo tikuwulalikira kwa inu ndi uwu: Mulungu ndiye kuwunika ndipo mwa Iye mulibe mdima konse. 6Tikanena kuti timayanjana naye, koma nʼkumayendabe mu mdima, tikunama ndipo sitikuchita choonadi. 7Koma tikamayenda mʼkuwunika, monga Iye ali mʼkuwunika, pamenepo timayanjana wina ndi mnzake, ndipo magazi a Yesu, Mwana wake, amatitsuka ndi kutichotsera tchimo lililonse.

Kuwulula Machimo ndi Kukhululukidwa

8Tikanena kuti tilibe tchimo, tikudzinyenga tokha ndipo mwa ife mulibe choonadi. 9Koma tikavomereza machimo athu, Iye ndi wokhulupirika ndi wolungama ndipo adzatikhululukira machimo athu, nadzatiyeretsa ndi kutichotsera chosalungama chilichonse. 10Ife tikanena kuti sitinachimwe, tikumutenga Mulungu kukhala wonama, ndipo Mawu ake sali mwa ife.