尼希米記 3 – CCBT & CCL

Chinese Contemporary Bible (Traditional)

尼希米記 3:1-32

重建耶路撒冷的城牆

1於是,大祭司以利亞實及其他祭司一起重建羊門,將它獻給上帝,又安上門。他們重建城牆,一直建到哈米亞樓和哈楠業樓,並將它獻給上帝。

2下一段由耶利哥人修建。

再下一段由音利的兒子撒刻修建。

3哈西拿的子孫修建魚門,架上橫樑,安上門,裝上門閂和門鎖。

4再下一段由哈哥斯的孫子、烏利亞的兒子米利末修築。

再下一段由米示薩別的孫子、比利迦的兒子米書蘭修築。

再下一段由巴拿的兒子撒督修築。

5再下一段由提哥亞人修築,但他們的貴族不肯做督工所分派的工作。

6巴西亞的兒子耶何耶大比所玳的兒子米書蘭修築古門,架上橫樑,安上門,裝上門閂和門鎖。

7再下一段由基遍米拉提米倫雅頓和其他基遍人,以及河西省省長管轄的米斯巴人修築。

8再下一段由哈海雅的兒子金匠烏薛修築。

再下一段由製造香料的哈拿尼雅修築,他們修築耶路撒冷的城牆,直到寬牆。

9再下一段由管理半個耶路撒冷戶珥的兒子利法雅修築。

10接下來,哈路抹的兒子耶大雅修築他房子對面的那一段。

再下一段由哈沙尼的兒子哈突修築。

11哈琳的兒子瑪基雅巴哈·摩押的兒子哈述修築另一段城牆,包括爐樓。

12再下一段由哈羅黑的兒子、管理另一半耶路撒冷沙龍和他的女兒們修築。

13哈嫩撒挪亞的居民修築谷門,安上門,裝上門閂和門鎖,之後又修建城牆四百四十五米,直到糞廠門。

14利甲的兒子、管理伯·哈基琳瑪基雅修築糞廠門,修好後安上門,裝上門閂和門鎖。

15各荷西的兒子、管理米斯巴沙崙修築泉門,修好後蓋上門頂,安上門,裝上門閂和門鎖。他還從靠近御花園的西羅亞池的城牆,一直修到大衛城下來的臺階處。

16再下一段由押蔔的兒子、管理半個伯·夙尼希米修築,他一直修到大衛墓地對面,遠至人工池和勇士堂。

修築城牆的利未人

17再下一段由巴尼的兒子利宏帶領的利未人修築。

接下來,管理半個基伊拉哈沙比雅修築了自己的轄區。

18再下一段由他的同族兄弟、管理另一半基伊拉希拿達的兒子巴瓦伊修築。

19再下一段由耶書亞的兒子、管理米斯巴以謝修築,他從斜坡對面修到城牆轉角的兵器庫。

20再下一段由薩拜的兒子巴錄修築,他從城牆轉角修到以利亞實大祭司的家門口。

21再下一段由哈哥斯的孫子、烏利亞的兒子米利末修築,他從以利亞實家門口修到以利亞實家的盡頭。

修築城牆的祭司

22再下一段由住在周圍郊區的祭司修築。

23接下來,便雅憫哈述修築自家對面的那一段。

再接下來,亞南尼的孫子、瑪西雅的兒子亞撒利雅修築自家旁邊的那一段。

24再下一段由希拿達的兒子賓內修築,他從亞撒利雅的房子修到城牆的轉角。

25-26再接下來,烏賽的兒子巴拉修築了城牆轉角的對面和護衛院附近上宮凸出的城樓。

再下一段由巴錄的兒子毗大雅與住在俄斐勒的殿役修築,他們修到東面的水門對面和凸出的城樓那裡。

其他修築的人

27再下一段由提哥亞人修築,他們從凸出來的大城樓對面修到俄斐勒的城牆。

28接下來,祭司修築了馬門以北的城牆,他們各自修築自家對面的部分。

29再接下來,音麥的兒子撒督修築自家對面的那一段。

再下一段由看守東門的、示迦尼的兒子示瑪雅修築。

30再下一段由示利米雅的兒子哈拿尼雅薩拉的第六個兒子哈嫩修築。

接下來,比利迦的兒子米書蘭修築自家對面的那一段。

31再下一段由金匠瑪基雅修築,他修到哈米弗甲門對面的殿役和商人的房子,直到城的角樓。

32金匠和商人修築從城的角樓到羊門的那一段。

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Nehemiya 3:1-32

Anthu Omanga Makoma a Yerusalemu

1Pambuyo pake Eliyasibu mkulu wa ansembe ndi ansembe anzake anayamba kugwira ntchito ndipo anamanganso Chipata cha Nkhosa. Iwo anachipatulira Mulungu ndipo anayika zitseko zake. Khoma limene analipatula linafika mpaka pa Nsanja ya Zana ndi Nsanja ya Hananeli. 2Anthu a ku Yeriko anamanga chigawo china pambali pake ndipo Zakuri mwana wa Imuri anamanga chigawo chinanso choyandikana nawo.

3Chipata cha Nsomba chinamangidwanso ndi ana a fuko la Hasena. Iwo anayika mitanda yake ndi zitseko, zotsekera zake, ndi mipiringidzo yake. 4Meremoti mwana wa Uriya, mwana wa Hakozi, anakonza chigawo choyandikana nacho. Motsatana naye, Mesulamu mwana wa Berekiya, mwana wa Mesezabeli anakonza chigawo china. Pambali pake, Zadoki mwana wa Baana anakonzanso chigawo china. 5Pambali pa iwowa anthu a ku Tekowa anakonza chigawo china. Koma wolemekezeka awo anakana kugwira ntchito imene akuluakulu awo anawapatsa.

6Chipata cha Yesana chinakonzedwa ndi Yoyada mwana wa Paseya ndi Mesulamu mwana wa Besodeya. Iwo anayika mitanda yake ndi kuyika zitseko, zotsekera zake ndi mipiringidzo yake. 7Pambali pawo Melatiya Mgibeyoni ndi Yadoni Mmerenoti ndiponso anthu a ku Gibiyoni ndi a ku Mizipa anakonza chigawo chawo mpaka ku nyumba ya bwanamkubwa wa chigawo cha Patsidya pa Yufurate. 8Pambali pawo Uzieli mwana wa Harihaya wa mʼgulu amisiri osula golide anakonzanso chigawo china. Pambali pake Hananiya mmodzi mwa anthu oyenga mafuta onunkhira, anakonzanso chigawo china. Iwo anakonzanso Yerusalemu mpaka ku Khoma Lotambasuka. 9Refaya mwana wa Huri wolamulira theka la chigawo cha Yerusalemu anakonza chigawo china motsatana nawo. 10Kulumikiza ichi, Yedaya mwana wa Harumafi anakonza chigawo choyangʼanana ndi nyumba yake, ndipo Hatusi mwana wa Hasabaneya anakonzanso motsatana naye. 11Malikiya mwana wa Harimu ndi Hasubu mwana wa Pahati-Mowabu anakonzanso chigawo china ndiponso Nsanja ya Ngʼanjo. 12Salumu mwana wa Halohesi wolamulira theka la chigawo cha Yerusalemu, anakonzanso chigawo chotsatana nawo mothandizidwa ndi ana ake akazi.

13Chipata cha ku chigwa chinakonzedwa ndi Hanuni ndi anthu okhala ku Zanowa. Iwo anachimanganso ndi kuyika zitseko zake ndi zotsekera ndi mipiringidzo yake. Iwo anakonzanso khoma lotalika mamita 450 mpaka ku Chipata cha Zinyalala.

14Chipata cha Zinyalala chinakonzedwa ndi Malikiya mwana wa Rekabu, wolamulira chigawo cha Beti-Hakeremu. Iye anachimanganso ndi kuyika zitseko zake, zotsekera zake ndi mipiringidzo.

15Chipata cha Kasupe chinakonzedwa ndi Saluni mwana wa Koli-Hoze, wolamulira chigawo cha Mizipa. Iye anachimanganso ndi kuyikanso denga ndiponso zitseko, zotsekera ndi mipiringidzo yake. Iye anakonzanso khoma la Dziwe la Siloamu limene lili pafupi ndi munda wa mfumu mpaka ku makwerero otsikira potuluka mzinda wa Davide. 16Pambali pa iyeyo, Nehemiya mwana wa Azibuki, wolamulira theka la chigawo cha Beti Zuri anakonza chigawo china mpaka kumalo oyangʼanana ndi manda a Davide, mpaka ku dziwe lokumba ndi ku nyumba ya anthu ankhondo.

17Pambali pake Alevi anakonza chigawo china, ndipo mtsogoleri wawo anali Rehumi mwana wa Bani. Pambali pa iye Hasabiya wolamulira theka la chigawo cha Keyila anagwira ntchito ku chigawo chake. 18Pambuyo pa iyeyu abale awo anapitiriza kukonza, ndipo mtsogoleri wawo anali Bawai mwana wa Henadadi, wolamulira theka lina la chigawo cha Keyila. 19Motsatana naye Ezeri mwana wa Yesuwa, wolamulira Mizipa anakonza chigawo chinanso choyangʼanana ndi chikweza chofikira ku nyumba yosungira zida za nkhondo pa ngodya. 20Motsatana naye, Baruki mwana wa Zakai anakonzanso chigawo china kuchokera pa ngodya mpaka pa chitseko cha nyumba ya Eliyasibu mkulu wa ansembe. 21Motsatana naye, Meremoti mwana wa Uriya, mwana wa Hakozi anakonzanso chigawo china kuchokera ku chitseko cha nyumba ya Eliyasibu mpaka kumapeto kwake.

22Pambuyo pake ansembe okhala ku chidikha anakonzanso chigawo china. 23Pambuyo pawo, Benjamini ndi Hasubu anakonza kutsogolo kwa nyumba zawo. Ndipo motsatana nawo, Azariya mwana wa Maaseya mwana wa Ananiya, anakonza chigawo choyangʼanana ndi nyumba zawo. 24Motsatana naye, Binuyi mwana wa Henadadi anakonzanso chigawo china, kuchokera pa nyumba ya Azariya kukafika potsirizira pa ngodya. 25Palali mwana Uzai anakonza chigawo china choyangʼanana ndi ngodya ndi nsanja yotuluka pa nyumba yapamwamba ya mfumu ku bwalo la alonda. Motsatana naye, Pedaya mwana wa Parosi, 26ndi otumikira mʼNyumba ya Mulungu amene amakhala pa khoma la Ofeli anakonza chigawo china mpaka pa malo oyangʼanana ndi Chipata cha Madzi kuloza kummawa ndiponso nsanja yayitali ija. 27Motsatana nawo, anthu a ku Tekowa anakonzanso chigawo china choyangʼanana ndi nsanja ija yayikulu ndi yayitali mpaka ku khoma la Ofeli.

28Kuyambira ku Chipata cha Akavalo anakonza ndi ansembe ena ndipo aliyense amakonza khoma loyangʼanana ndi nyumba yake. 29Motsatana nawo, Zadoki mwana wa Imeri anakonza chigawo china choyangʼanana ndi nyumba yake. Motsatana naye, Semeya mwana wa Sekaniya, mlonda wa Chipata cha Kummawa, anakonzanso khoma. 30Hananiya mwana wa Selemiya ndiponso Hanuni mwana wachisanu ndi chimodzi wa Zalafi anakonza chigawo china. Motsatana naye, Mesulamu mwana wa Berekiya anakonza chigawo choyangʼanana ndi chipinda chake. 31Motsatana naye, Malikiya mmodzi mwa amisiri a golide anakonza chigawo china mpaka ku nyumba ya atumiki a ku Nyumba ya Mulungu ndiponso ku nyumba ya anthu amalonda moyangʼanana ndi chipata cha Mifikade ndiponso mpaka pa chipinda chapamwamba chapangodya. 32Ndipo pakati pa chipinda chapamwamba chapangodya ndi Chipata cha Nkhosa anakonza ndi amisiri a golide ndi anthu amalonda.