诗篇 131 – CCB & CCL

Chinese Contemporary Bible (Simplified)

诗篇 131:1-3

第 131 篇

全心仰望上帝

大卫上圣殿朝圣之诗。

1耶和华啊,

我的心不狂傲,

我的眼目也不高傲;

我不敢涉猎太伟大、太奇妙的事。

2我的心灵平静安稳,

如同母亲身边断奶的孩子,

我的心灵如同断奶的孩子。

3以色列啊,

你要仰望耶和华,

从现在直到永远。

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Masalimo 131:1-3

Salimo 131

Nyimbo yoyimba pokwera ku Yerusalemu. Salimo la Davide.

1Inu Yehova, mtima wanga siwodzikuza,

maso anga siwonyada;

sinditengeteka mtima

ndi zinthu zapamwamba ndi zodabwitsa.

2Koma moyo wanga ndawutontholetsa

ndi kuwukhalitsa chete ngati mwana amene amayi ake amuletsa kuyamwa,

moyo wanga mʼkati mwanga uli ngati mwana amene amuletsa kuyamwa.

3Yembekeza Yehova, iwe Israeli,

kuyambira tsopano mpaka muyaya.