诗篇 126 – CCB & CCL

Chinese Contemporary Bible (Simplified)

诗篇 126:1-6

第 126 篇

被掳者归回的喜乐

上圣殿朝圣之诗。

1耶和华带领被掳者归回耶路撒冷的时候,

我们犹如在梦中。

2我们笑声不止,欢呼歌唱。

列邦都说:

“耶和华为他们成就了伟大的事。”

3耶和华实在为我们成就了伟大的事,

我们充满了喜乐。

4耶和华啊,

求你恢复我们的繁荣,

就像干旱的南地重现溪流。

5含泪撒种的必欢呼着收割。

6含泪出去撒种的必欢呼着带回禾捆。

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Masalimo 126:1-6

Salimo 126

Nyimbo yoyimba pokwera ku Yerusalemu.

1Yehova atabwezera akapolo ku Ziyoni,

tinali ngati amene akulota.

2Pakamwa pathu panadzaza ndi kuseka;

malilime athu ndi nyimbo zachimwemwe.

Pamenepo kunanenedwa pakati pa anthu kuti,

“Yehova wawachitira zinthu zazikulu.”

3Yehova watichitira zinthu zazikulu,

ndipo tadzazidwa ndi chimwemwe.

4Tibwezereni madalitso athu, Inu Yehova,

monga mitsinje ya ku Negevi.

5Iwo amene amafesa akulira,

adzakolola akuyimba nyimbo zachimwemwe.

6Iye amene amayendayenda nalira,

atanyamula mbewu yokafesa,

adzabwerera akuyimba nyimbo zachimwemwe,

atanyamula mitolo yake.