诗篇 122 – CCB & CCL

Chinese Contemporary Bible (Simplified)

诗篇 122:1-9

第 122 篇

为耶路撒冷祷告

大卫上圣殿朝圣之诗。

1人们对我说:

“让我们去耶和华的殿吧!”

我感到欢喜。

2耶路撒冷啊,

我们踏进你的城门了。

3耶路撒冷是一座整齐坚固的城。

4以色列各支派,耶和华的子民,

都遵照祂赐的法度去那里称谢祂。

5那里有审判的王座,

就是大卫家的王座。

6要为耶路撒冷的和平祷告,

愿爱这城的人亨通。

7耶路撒冷啊!

愿你城内有平安,

你的宫里有安宁,

8为了我的亲人和朋友,

我要祈求平安临到你。

9为了我们的上帝耶和华的殿,

我要为你求福祉。

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Masalimo 122:1-9

Salimo 122

Salimo la Davide. Nyimbo yoyimba pokwera ku Yerusalemu.

1Ndinakondwera atandiwuza kuti,

“Tiyeni ku nyumba ya Yehova.”

2Mapazi athu akuyima mʼzipata

zako, Iwe Yerusalemu.

3Yerusalemu anamangidwa ngati mzinda

umene uli wothithikana pamodzi.

4Kumeneko ndiye kumene kumapita mafuko,

mafuko a Yehova,

umboni wa kwa Israeli,

kuti atamande dzina la Yehova.

5Kumeneko anayikako mipando yaufumu yachiweruzo,

mipando yaufumu ya nyumba ya Davide.

6Pemphererani mtendere wa Yerusalemu:

“Iwo amene amakukonda iwe zinthu ziwayendere bwino.

7Mukhale mtendere mʼkati mwa makoma ako,

ndipo mʼnyumba zako zaufumu mukhale chitetezo.”

8Chifukwa cha abale anga ndi abwenzi anga

ndidzati, “Mtendere ukhale mʼkati mwako.”

9Chifukwa cha Nyumba ya Yehova Mulungu wathu,

ndidzakufunira zabwino.