Забур 127 – CARSA & CCL

Священное Писание (Восточный перевод), версия с «Аллахом»

Забур 127:1-6

Песнь 127

Песнь восхождения.

1Благословен всякий, кто боится Вечного

и ходит Его путями!

2Ты будешь есть плоды своего труда;

благословение и процветание будут у тебя.

3Жена твоя будет как плодовитая лоза

в твоём доме,

твои дети будут как ветви маслин

вокруг твоего стола.

4Так будет благословлён человек,

боящийся Вечного.

5Да благословит тебя Вечный с Сиона,

да увидишь ты процветание Иерусалима

во все дни своей жизни

6и да увидишь своих внуков.

Мир Исраилу!

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Masalimo 127:1-5

Salimo 127

Nyimbo yoyimba pokwera ku Yerusalemu. Salimo la Solomoni.

1Yehova akapanda kumanga nyumba,

omanga nyumbayo agwira ntchito pachabe.

Yehova akapanda kulondera mzinda,

mlonda akanangolondera pachabe.

2Mumangodzivuta nʼkulawirira mmamawa

ndi kusagona msanga madzulo,

kuvutikira chakudya choti mudye,

pakuti Iye amapereka tulo kwa amene amawakonda.

3Ana ndiye cholowa chochokera kwa Yehova,

ana ndi mphotho yochokera kwa Iye.

4Ana a pa unyamata ali ngati mivi mʼmanja

mwa munthu wankhondo.

5Wodala munthu

amene motengera mivi mwake mwadzaza.

Iwo sadzachititsidwa manyazi

pamene alimbana ndi adani awo pa zipata.