Аюб 25 – CARSA & CCL

Священное Писание (Восточный перевод), версия с «Аллахом»

Аюб 25:1-6

Третья речь Билдада

1Тогда ответил Билдад из Шуаха:

2– Держава и страх у Аллаха,

творящего мир в высотах Своих.

3Можно ли счесть Его небесные воинства?

И над кем Его свет не светит?

4Так может ли смертный быть праведен перед Аллахом

и рождённый женщиной – чист?

5Ведь если даже луна не светла,

и звёзды нечисты в Его глазах,

6то тем более человек, который лишь тля,

и смертный, который лишь червь!

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Yobu 25:1-6

Mawu a Bilidadi

1Apo Bilidadi wa ku Suki anayankha kuti,

2“Ulamuliro ndi kuopsa ndi za Mulungu,

Iye amakhazikitsa bata mu ufumu wake kumwambako.

3Kodi magulu ake ankhondo nʼkuwerengeka?

Kodi kuwala kwake sikuwalira ndani?

4Kodi munthu angakhale bwanji wolungama pamaso pa Mulungu?

Kodi munthu wobadwa mwa mayi angakhale wangwiro?

5Ngati mwezi sutha kuwala kwenikweni,

ndipo nyenyezi sizitha kuwala pamaso pake,

6nanji tsono munthu amene ali ngati mphutsi,

mwana wa munthu amene ali ngati nyongolotsi!”