Забур 114 – CARS & CCL

Священное Писание

Забур 114:1-9

Песнь 114Песнь 114 В тексте оригинала песни 114 и 115 объединены в одну песнь.

1Я люблю Вечного,

потому что Он услышал мой голос, мои моления.

2Он услышал меня,

и потому буду призывать Его, пока жив.

3Узы смерти оплели меня,

адские муки постигли меня;

я познал бедствие и скорбь.

4Тогда я призвал имя Вечного:

«О Вечный, умоляю, спаси меня!»

5Вечный милостив и праведен;

милосерден Бог наш.

6Хранит Вечный простодушных;

когда я изнемогал, Он спас меня.

7Возвратись, душа моя, в свой покой,

потому что Вечный был благ к тебе.

8Вечный, Ты избавил душу мою от смерти,

глаза мои – от слёз

и ноги мои – от падения.

9Буду ходить перед Вечным

на земле живых.

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Masalimo 114:1-8

Salimo 114

1Pamene Israeli anatuluka mu Igupto,

nyumba ya Yakobo kuchoka ku mtundu wa anthu a chiyankhulo chachilendo,

2Yuda anasanduka malo opatulika a Mulungu,

Israeli anasanduka ufumu wake.

3Nyanja inaona ndi kuthawa,

mtsinje wa Yorodani unabwerera mʼmbuyo;

4mapiri analumphalumpha ngati nkhosa zazimuna,

timapiri ngati ana ankhosa.

5Nʼchifukwa chiyani iwe unathawa?

iwe mtsinje wa Yorodani unabwereranji mʼmbuyo?

6inu mapiri, munalumphalumphiranji ngati nkhosa zazimuna,

inu timapiri, ngati ana ankhosa?

7Njenjemera pamaso pa Ambuye iwe dziko lapansi,

pamaso pa Mulungu wa Yakobo,

8amene anasandutsa thanthwe kukhala chitsime,

thanthwe lolimba kukhala akasupe a madzi.