Dwom 19
Dawid dwom.
1Ɔsoro ka Onyankopɔn anuonyam!
Wim pae mu ka ne nsa ano adwuma,
2Da biara, wɔkasa;
anadwo biara, wɔda nimdeɛ adi.
3Wonni ɔkasa, wɔnnka nsɛm;
wɔnnte wɔn nne.
4Wɔn nne akodu asase so mmaa nyinaa,
na wɔn nsɛm nso akodu asase ano.
Onyankopɔn asi ntamadan ama owia wɔ ɔsoro hɔ.
5Ɛte sɛ ayeforokunu a ofi ne pia mu,
te sɛ ɔbran a ne ho pere no sɛ obetu ne mmirika.
6Epue wɔ ɔsoro fa baabi
na atwa ne ho akosi ano;
biribiara nsiw ne hyew ho kwan.
7Awurade mmara yɛ pɛ,
ɛkanyan ɔkra no.
Ahotoso wɔ Awurade nhyehyɛe mu,
ɛma nea onnim nyansa hu nyansa.
8Awurade ahyɛde teɛ;
ɛma koma mu anigye.
Awurade ɔhyɛ nsɛm mu da hɔ;
na ebue ani.
9Awurade suro yɛ kronkron,
ɛte hɔ daa.
Awurade mmara nsɛm yɛ nokware
na ne nyinaa teɛ.
10Ɛsom bo sen sikakɔkɔɔ
ɛsen sikakɔkɔɔ kann;
ɛyɛ dɛ sen ɛwo,
ɛsen ɛwo a efi ɛwokyɛm mu.
11Wɔnam so bɔ wo somfo kɔkɔ se,
sodi so akatua yɛ bebree.
12Hena na ohu nʼankasa mfomso?
Fa me mfomso a ahintaw kyɛ me.
13Bɔ wʼakoa ho ban fi ɔboayɛ bɔne ho,
na anhyɛ me so.
Ɛno na ɛbɛma madi bem,
a merenni fɔ wɔ bɔne akɛse ho.
14Ma mʼanom nsɛm ne me koma mu adwene
nyɛ nea ɛsɔ wʼani, Awurade
me Botan ne me Gyefo.
Salimo 19
Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Salimo la Davide.
1Zakumwamba zimalengeza za ulemerero wa Mulungu;
thambo limalalikira ntchito za manja ake.
2Tsiku ndi tsiku zimayankhula mawu ambiri,
usiku ndi usiku zimaonetsa poyera nzeru.
3Palibe kuyankhula, palibe mawu aliwonse;
liwu lawo silimveka.
4Koma uthenga wawo umapita pa dziko lonse lapansi,
mawuwo amafika mpaka
kumalekezero a dziko lapansi.
5Dzuwa lili ngati mkwatibwi wobwera kuchokera ku nsanja yake,
ngati katswiri wokondwerera kuthamanga pa mpikisano.
6Limatuluka kuyambira mbali ina ya thambo
ndi kuzungulira mpaka mbali inanso;
palibe chinthu chotha kupewa kutentha kwake.
7Lamulo la Yehova ndi langwiro,
kutsitsimutsa moyo.
Maumboni a Yehova ndi odalirika,
amapereka nzeru kwa wopanda nzeru.
8Malangizo a Yehova ndi olungama,
amapereka chimwemwe mu mtima.
Malamulo a Yehova ndi onyezimira,
amapereka kuwala.
9Kuopa Yehova ndiye chinthu changwiro,
chimakhala mpaka muyaya.
Maweruzo a Yehova ndi owona
ndipo onse ndi olungama;
10ndi a mtengowapatali kuposa golide,
kuposa golide weniweni;
ndi otsekemera kuposa uchi,
kuposa uchi wochokera pa chisa chake.
11Mtumiki wanu amachenjezedwa nawo;
powasunga pali mphotho yayikulu.
12Ndani angathe kudziwa zolakwa zake?
Mundikhululukire zolakwa zanga zobisika.
13Muteteze mtumiki wanunso ku machimo ochita akudziwa;
iwo asandilamulire.
Kotero ndidzakhala wosalakwa,
wopanda mlandu wa tchimo lalikulu.
14Mawu a mʼkamwa mwanga ndi zolingalira za mu mtima mwanga
zikhale zokondweretsa pamaso panu,
Inu Yehova, Thanthwe langa ndi Mpulumutsi wanga.