Nnwom 112 – AKCB & CCL

Akuapem Twi Contemporary Bible

Nnwom 112:1-10

Dwom 112

1Monkamfo Awurade.

Nhyira nka onipa a osuro Awurade

na onya nʼahyɛde mu anigye pii.

2Ne mma bɛyɛ atumfo wɔ asase no so;

atreneefo awo ntoatoaso benya nhyira.

3Ahonya ne sika wɔ ne fi,

na ne trenee tena hɔ daa.

4Sum mu mpo hann pue ma nnipa a wɔteɛ,

ma ɔdomfo, mmɔborɔhunufo ne ɔnokwafo.

5Yiyedi bɛba wɔn a wɔn tirim yɛ mmerɛw na wɔde fɛm kwa,

wɔn a wɔde atɛntrenee yɛ wɔn nneɛma no so.

6Ampa ara ɔrenhinhim da biara da;

wɔbɛkae onipa trenee daa.

7Ɔte asɛmmɔne a, ɛmmɔ no hu;

ne koma si pi wɔ Awurade mu ahotoso mu.

8Ne koma wɔ bammɔ, na onsuro;

awiei no ɔde nkonimdi behyia nʼatamfo.

9Ɔtow nʼakyɛde pete aman so ma ahiafo nea wohia,

nʼadɔe no tena hɔ daa;

wɔbɛkae wɔn daa na wɔahyɛ wɔn anuonyam.

10Omumɔyɛfo behu ama ayɛ no yaw,

ɔbɛtwɛre ne se na wafɔn;

omumɔyɛfo tirimpɔw bɛyɛ ɔkwa.

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Masalimo 112:1-10

Salimo 112

1Tamandani Yehova.

Wodala munthu amene amaopa Yehova,

amene amakondwera kwambiri ndi malamulo ake.

2Ana ake adzakhala amphamvu mʼdziko;

mʼbado wa olungama mtima udzadalitsidwa.

3Kulemera ndi chuma zili mʼnyumba yake,

ndipo chilungamo chake ndi chosatha.

4Ngakhale mu mdima kuwala kumatulukira olungama mtima;

wokoma mtima, wachifundo ndi wowongoka mtima.

5Zinthu zabwino zidzabwera kwa iye amene amapereka mowolowamanja ndi wokongoletsa mwaufulu,

amene amachita ntchito yake mwachilungamo.

6Ndithu sadzagwedezeka;

munthu wolungama sadzayiwalika mpaka muyaya.

7Saopa akamva zoyipa zimene zachitika;

mtima wake ndi wokhazikika ndipo amadalira Yehova.

8Mtima wake ndi wotetezedwa, sadzakhala ndi mantha;

potsiriza pake adzayangʼana adani ake mwachipambano.

9Wopereka mphatso zake mowolowamanja kwa osauka,

chilungamo chake chimanka mpaka muyaya;

nyanga yake idzakwezedwa mwaulemu.

10Munthu woyipa adzaona zimenezi ndipo adzapsa mtima;

adzakukuta mano ake ndipo adzasungunuka.

Zolakalaka za anthu oyipa sizidzachitika konse.