Hiob 41 – AKCB & CCL

Akuapem Twi Contemporary Bible

Hiob 41:1-34

1“So wubetumi de darewa atwe ɔdɛnkyɛmmirampɔn

anaa wubetumi de hama akyekyere ne tɛkrɛma?

2So wubetumi de hama afa ne hwenem,

anaasɛ wubetumi de darewa aso nʼabogye mu?

3Ɔbɛkɔ so asrɛ wo sɛ hu no mmɔbɔ ana?

Ɔne wo bɛkasa brɛoo ana?

4Ɔbɛpene ne wo ayɛ apam

ama wode no ayɛ wʼakoa afebɔɔ ana?

5Wubetumi de no ayɛ abɛbɛ te sɛ anomaa

anaa wubetumi asa no hama de no ama wo mmabea?

6So aguadifo bɛpɛ sɛ wode no bedi nsesagua?

Wɔbɛkyekyɛ ne mu ama aguadifo ana?

7Wubetumi de mpeaw awowɔ ne were mu

anaasɛ wode mpataa mpɛmɛ bɛwowɔ ne ti ho?

8Wode wo nsa ka no a,

wobɛkae sɛnea ɔbɛwosow ne ho, nti worenyɛ saa bio!

9Ɔkwan biara nni hɔ a wobɛfa so akyere no;

ani a ɛbɔ ne so kɛkɛ no ma nnipa dwudwo.

10Obiara ntumi nsi ne bo nhwanyan no.

Afei hena na obetumi ne me adi asi?

11Hena na mede no ka a ɛsɛ sɛ mitua?

Biribiara a ɛhyɛ ɔsoro ase no yɛ me de.

12“Me werɛ remfi sɛ mɛka nʼakwaa,

nʼahoɔden ne ne bɔbea fɛfɛ no ho asɛm.

13Hena na obetumi aworɔw ne ho ahama,

na hena na ɔde nnareka bɛkɔ ne ho?

14Hena na obetumi abue nʼabogye,

a ɛse a ɛyɛ hu ayɛ no ma no?

15Nʼakyi wɔ bona a ɛsesa so,

ɛtetare so a ɔkwan nna mu koraa;

16sɛnea ɛtetare so fa no nti,

mframa biara mfa ntam.

17Ɛtoatoa mu denneennen a

emu ntumi ntetew.

18Sɛ ɔnwansi a, ɛpepa gya;

nʼaniwa aba te sɛ adekyeenim hann.

19Agyatɛn turuw fi nʼanom

na nsramma turuturuw fi mu.

20Wusiw sen fi ne hwene mu

te sɛ ɔsɛn a esi gya so.

21Ne home ma gyabiriw ano sɔ,

na ogyaframa tu fi nʼanom.

22Ne kɔn mu wɔ ahoɔden ankasa;

wɔn a wohu no no aba mu bu.

23Ne were a abubu agu so no yɛ peperee;

ayɛ pemee a ɛnka ne ho.

24Ne koko so yɛ den sɛ ɔbotan

ɛyɛ den sɛ awiyammo.

25Sɛ ɔsɔre a, ahoɔdenfo bɔ huboa;

sɛ ɔwosow ne ho a woguan.

26Afoa wɔ no a, ɛnka no,

peaw, pɛmɛ ne agyan nso saa ara.

27Ɔfa dade sɛ wura bi

na kɔbere mfrafrae te sɛ dua a awu bi ma no.

28Agyan mma no nguan;

ahwimmo mu aboa yɛ ntɛtɛ ma no.

29Kontibaa te sɛ sare wɔ nʼani so;

na ɔserew pɛmɛ nnyigyei.

30Abon a ano yɛ nnam tuatua ne yafunu so.

Ɔtwe ne ho ase wɔ fam fa dontori mu a, eyiyi akam.

31Ɔma bun mu huru sɛ nsu a ɛwɔ ɛsɛn mu

na onunu po mu sɛ srade a ɛwɔ kuku mu.

32Nea ɔbɛfa no, ɛhɔ nsu no pa yerɛw yerɛw;

na obi besusuw sɛ po bun adan ayɛ dwen.

33Asase so biribiara ne no nsɛ.

Ɔyɛ abɔde a onsuro hwee.

34Ommu wɔn a wɔyɛ ahantan no mu biara;

ɔyɛ wɔn a wɔyɛ ahomaso no nyinaa so hene.”

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Yobu 41:1-34

1“Kodi ungathe kukoka ngʼona ndi mbedza ya nsomba

kapena kukanikiza lilime lake pansi ndi chingwe?

2Kodi ungathe kumanga chingwe mʼmphuno mwake,

kapena kubowola nsagwada zake ndi mbedza?

3Kodi ngʼonayo idzakupempha kuti uyichitire chifundo?

Kodi idzakuyankhula ndi mawu ofatsa?

4Kodi idzachita nawe mgwirizano

kuti uyisandutse kapolo wako mpaka muyaya?

5Kodi udzasewera nayo ngati mbalame,

kapena kuyimangirira kuti atsikana ako asewere nayo?

6Kodi anthu adzayitsatsa malonda?

Nanga amalondawo nʼkugawanagawana nyama yake kuti akagulitse?

7Kodi chikopa chake ungathe kuchilasa ndi zisonga,

kapena kubowola mutu wake ndi nthungo zophera nsomba?

8Ukayiputa udziwe kuti pali nkhondo,

ndipo iweyo sudzabwereranso.

9Chiyembekezo choti nʼkuyigonjetsa ndi chabodza;

kungoyiona kokha, ndithu iwe kumangodzigwera wekha.

10Palibe wolimba mtima kuti ndi kuyiputa.

Ndani angalimbe mtima kulimbana ndi Ine?

11Kodi ndani anandipatsa kanthu kuti ndimubwezere?

Zonse za pansi pa thambo ndi zanga.

12“Sindidzaleka kuyankhula za ziwalo zake za chirombocho,

za mphamvu zake ndiponso za maonekedwe a thupi lake.

13Ndani angasende chikopa chake?

Ndani angayiyandikire kuti abowole chikopa chake cholimbacho?

14Ndani angatsekule kukamwa kwake,

pakamwa pamene pazunguliridwa ndi mano ochititsa mantha?

15Kumsana kwake kuli mizere ya mamba

onga zishango zolumikizanalumikizana;

16Mambawo ndi olukanalukana

kotero kuti mpweya sungathe kulowa pakati pake.

17Ndi olumikizanalumikizana;

ndi omatirirana kwambiri kotero kuti sangathe kulekana.

18Kuyetsemula kwake kumatulutsa mbaliwali;

maso ake amawala ngati kuwala kwa mʼbandakucha.

19Mʼkamwa mwake mumatuluka nsakali zamoto ndipo

mumathetheka mbaliwali zamoto.

20Mʼmphuno mwake mumatuluka utsi

ngati wa mʼnkhali yowira yomwe ili pa moto wa bango.

21Mpweya wake umayatsa makala,

ndipo malawi amoto amatuluka mʼkamwa mwake.

22Mphamvu zake zili mʼkhosi mwake;

aliyense wokumana nayo amangoti njenjenje ndi mantha.

23Minyewa ya thupi lake ndi yolumikizana ndipo

ndi yokhwima kwambiri ndi yolimba.

24Pachifuwa pake ndi powuma ngati mwala,

ndi pa gwaa, ngati mwala wamphero.

25Ngʼonayo ikangovuwuka,

ndi anthu amphamvu omwe amaopa; amabwerera mʼmbuyo, kuthawa.

26Ngakhale ikanthidwe ndi lupanga, lupangalo silichita kanthu,

ngakhale mkondo, muvi ndi nthungo, zonse zimalephera.

27Chitsulo imachiyesa ngati phesi chabe

ndi mkuwa ngati chikuni chowola.

28Muvi sungathe kuyithawitsa,

miyala imene ayilasa nayo imangoyinyenyanyenya.

29Zibonga zimakhala ngati ziputu;

imangoseka pamene akuyibaya ndi nthungo.

30Mamba a ku mimba kwake ali ngati chopunthira chakunthwa ndipo

imasiya mkukuluzi mʼmatope ngati galeta lopunthira tirigu.

31Imagadutsa madzi ozama ngati madzi a mʼnkhali,

imachititsa nyanja kuti iwire ngati mbiya yoyengera mafuta.

32Kumbuyo kwake imasiya nthubwitubwi zambee,

kotero kuti munthu angaganize kuti nyanja yachita imvi.

33Pa dziko lapansi palibe china chofanana nacho,

nʼcholengedwa chopanda mantha.

34Chimanyoza nyama zina zonse;

icho chija ndi mfumu ya nyama zonse.”