Zaburi 97 – NEN & CCL

Kiswahili Contemporary Version (Neno: Bibilia Takatifu)

Zaburi 97:1-12

Zaburi 97

Mungu Mtawala Mkuu

197:1 Kut 15:18; Za 93:1; 96:10; 99:1; 96:11; Isa 24:23; 52:7Bwana anatawala, nchi na ifurahi,

visiwa vyote vishangilie.

297:2 Ay 22:14; Kut 19:9; Za 89:14Mawingu na giza nene vinamzunguka,

haki na hukumu ndio msingi wa kiti chake cha enzi.

397:3 Dan 7:10; Hab 3:5; Isa 9:19; Yoe 1:19; 2:3; Hab 3:5; 2Sam 22:9Moto hutangulia mbele zake

na huteketeza adui zake pande zote.

497:4 Ay 36:30; 2Sam 22:8; Za 18:7; 104:32; Ufu 6:12Umeme wake wa radi humulika dunia,

nchi huona na kutetemeka.

597:5 Za 46:2, 6; 22:14; Yos 3:11Milima huyeyuka kama nta mbele za Bwana,

mbele za Bwana wa dunia yote.

697:6 Za 50:6; 98:2; 19:1Mbingu zinatangaza haki yake,

na mataifa yote huona utukufu wake.

797:7 Kut 12:12; 20:4; Isa 37:18, 19; 42:17; Law 26:1; Kum 5:8; Yer 10:14; Ebr 1:6; Za 16:4Wote waabuduo sanamu waaibishwa,

wale wajisifiao sanamu:

mwabuduni yeye, enyi miungu yote!

897:8 Za 9:2; 48:11Sayuni husikia na kushangilia,

vijiji vya Yuda vinafurahi

kwa sababu ya hukumu zako, Ee Bwana.

997:9 Ay 34:29; Efe 1:21; Za 7:8; 47:9Kwa kuwa wewe, Ee Bwana, ndiwe Uliye Juu Sana kuliko dunia yote;

umetukuka sana juu ya miungu yote.

1097:10 Ay 28:28; Mit 2:8; Za 145:20; 31:23; 101:3; 37:28, 40; 34:7; Yer 15:21; 20:13; Dan 3:28; 6:16; 1Sam 2:9; Rum 12:9; 7:15; Amo 5:15Wale wanaompenda Bwana na wauchukie uovu,

kwa maana yeye hulinda maisha ya waaminifu wake

na kuwaokoa kutoka mkononi mwa mwovu.

1197:11 Ay 22:28; Za 11:5; 7:10Nuru huangaza wenye haki

na furaha kwa watu wanyofu wa moyo.

1297:12 Ay 22:19; Flp 4:4; Kut 3:15; Isa 41:16; Za 99:5; 104:34Furahini katika Bwana, ninyi mlio wenye haki,

lisifuni jina lake takatifu.

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Masalimo 97:1-12

Salimo 97

1Yehova akulamulira, dziko lapansi lisangalale;

magombe akutali akondwere.

2Mitambo ndi mdima waukulu zamuzungulira;

chilungamo ndi kuweruza molungama ndiwo maziko a mpando wake waufumu.

3Moto umapita patsogolo pake

ndi kunyeketsa amaliwongo kumbali zonse.

4Zingʼaningʼani zake zimawalitsa dziko lonse;

dziko lapansi limaona ndipo limanjenjemera.

5Mapiri amasungunuka ngati phula pamaso pa Yehova,

pamaso pa Ambuye a dziko lonse lapansi.

6Mayiko akumwamba amalengeza za chilungamo chake,

ndipo mitundu yonse ya anthu imaona ulemerero wake.

7Onse amene amalambira mafano osema amachititsidwa manyazi,

iwo amene amanyadira mafano;

mulambireni, inu milungu yonse!

8Ziyoni akumva ndipo akukondwera,

midzi ya Yuda ikusangalala

chifukwa cha maweruzo anu Yehova.

9Pakuti Inu Yehova ndi Wammwambamwamba pa dziko lonse lapansi;

ndinu wokwezeka kupambana milungu yonse.

10Iwo amene amakonda Yehova adane ndi zoyipa

pakuti Iye amayangʼanira miyoyo ya amene amamukhulupirira

ndipo amawapulumutsa mʼdzanja la anthu oyipa

11Kuwala kumafika pa anthu olungama,

ndi chimwemwe kwa olungama mtima.

12Kondwerani mwa Yehova Inu olungama

ndipo tamandani dzina lake loyera.