Zaburi 120 – NEN & CCL

Kiswahili Contemporary Version (Neno: Bibilia Takatifu)

Zaburi 120:1-7

Zaburi 120

Kuomba Msaada

Wimbo wa kwenda juu.

1120:1 2Sam 22:7; Za 18:1; 118:5Katika dhiki yangu namwita Bwana,

naye hunijibu.

2120:2 Za 31:18; 52:4Ee Bwana, uniokoe kutoka midomo ya uongo

na ndimi za udanganyifu.

3Atakufanyia nini,

au akufanyie nini zaidi, ewe ulimi mdanganyifu?

4120:4 Kum 32:23Atakuadhibu kwa mishale mikali ya shujaa,

kwa makaa yanayowaka ya mti wa mretemu.

5120:5 Mwa 25:13; 2:10; Yer 2:10; 49:28; 1Sam 25:1Ole wangu kwa kuwa naishi Mesheki,

kwamba naishi katikati ya hema za Kedari!

6Nimeishi muda mrefu mno

miongoni mwa wale wanaochukia amani.

7Mimi ni mtu wa amani;

lakini ninaposema, wao wanataka vita.

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Masalimo 120:1-7

Salimo 120

Nyimbo yoyimba pokwera ku Yerusalemu.

1Ndimafuwulira kwa Yehova mʼmasautso anga,

ndipo Iye amandiyankha.

2Pulumutseni Yehova ku milomo yabodza,

ndi kwa anthu achinyengo.

3Kodi adzakuchitani chiyani,

ndipo adzawonjezerapo zotani, inu anthu achinyengo?

4Adzakulangani ndi mivi yakuthwa ya munthu wankhondo,

ndi makala oyaka a mtengo wa tsanya.

5Tsoka ine kuti ndimakhala ku Mesaki,

kuti ndimakhala pakati pa matenti a ku Kedara!

6Kwa nthawi yayitali ndakhala pakati

pa iwo amene amadana ndi mtendere.

7Ine ndine munthu wamtendere;

koma ndikamayankhula, iwo amafuna nkhondo.