詩篇 127 – JCB & CCL

Japanese Contemporary Bible

詩篇 127:1-5

127

1主が建てたものでなければ、家を建ててもむだです。

主に町を守っていただかないのなら、

見張りが立つ意味もありません。

2暮らしを支えるために朝早くから夜遅くまで

身を粉にして働いたとしても、

それが何になるでしょう。

主は、愛する者には必要な休息を

与えようとなさるお方です。

3子どもたちは主からの贈り物であり、報いです。

4若いうちに生まれた子どもは、

身を守る鋭い矢のようです。

5矢筒が矢で満ちている人は幸せです。

敵と論争するときにも、

助けを得ることができるからです。

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Masalimo 127:1-5

Salimo 127

Nyimbo yoyimba pokwera ku Yerusalemu. Salimo la Solomoni.

1Yehova akapanda kumanga nyumba,

omanga nyumbayo agwira ntchito pachabe.

Yehova akapanda kulondera mzinda,

mlonda akanangolondera pachabe.

2Mumangodzivuta nʼkulawirira mmamawa

ndi kusagona msanga madzulo,

kuvutikira chakudya choti mudye,

pakuti Iye amapereka tulo kwa amene amawakonda.

3Ana ndiye cholowa chochokera kwa Yehova,

ana ndi mphotho yochokera kwa Iye.

4Ana a pa unyamata ali ngati mivi mʼmanja

mwa munthu wankhondo.

5Wodala munthu

amene motengera mivi mwake mwadzaza.

Iwo sadzachititsidwa manyazi

pamene alimbana ndi adani awo pa zipata.