Yobu 25 – CCL & JCB

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Yobu 25:1-6

Mawu a Bilidadi

1Apo Bilidadi wa ku Suki anayankha kuti,

2“Ulamuliro ndi kuopsa ndi za Mulungu,

Iye amakhazikitsa bata mu ufumu wake kumwambako.

3Kodi magulu ake ankhondo nʼkuwerengeka?

Kodi kuwala kwake sikuwalira ndani?

4Kodi munthu angakhale bwanji wolungama pamaso pa Mulungu?

Kodi munthu wobadwa mwa mayi angakhale wangwiro?

5Ngati mwezi sutha kuwala kwenikweni,

ndipo nyenyezi sizitha kuwala pamaso pake,

6nanji tsono munthu amene ali ngati mphutsi,

mwana wa munthu amene ali ngati nyongolotsi!”

Japanese Contemporary Bible

ヨブ 記 25:1-6

25

ビルダデのことば

1シュアハ人ビルダデの三度目の返答。

2「神は力のある、恐るべきお方だ。

神は天で平和をつくる。

3だれに、おびただしい御使いの数を

数えることができるだろう。

神の光は地をすみずみまで照らす。

4人にすぎない者が、神の前に立ち、

自分は正しいと主張できようか。

胸を張って、自分は潔白だと言いきれる者は、

この世界にただの一人もいない。

5神の栄光はあまりにもまばゆく、

月や星でさえ比べることもできない。

6まして、神の目には虫けらにすぎない人間は、

なおさらのことだ。」