Masalimo 85 – CCL & KLB

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Masalimo 85:1-13

Salimo 85

Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Salimo la ana a Kora.

1Yehova munakomera mtima dziko lanu;

munabwezeretsa ulemerero wa Yakobo.

2Munakhululukira mphulupulu za anthu anu

ndi kuphimba machimo awo onse.

Sela

3Munayika pambali ukali wanu wonse

ndi kutembenuka kuchoka ku mkwiyo wanu woopsa.

4Tibwezeretseninso mwakale Inu Mulungu Mpulumutsi wathu,

ndipo mutichotsere mkwiyo wanu.

5Kodi mudzatikwiyira mpaka liti?

Kodi mudzapitiriza kukwiya pa mibado yathu yonse?

6Kodi simudzatitsitsimutsanso,

kuti anthu anu asangalale mwa Inu?

7Tionetseni chikondi chanu chosatha, Inu Yehova,

ndipo tipatseni chipulumutso chanu.

8Ndidzamvetsera zimene Yehova Mulungu adzanena;

Iye amalonjeza mtendere kwa anthu ake, oyera mtima ake,

koma musawalole kuti abwerere ku zopusa.

9Ndithu chipulumutso chake chili pafupi ndi iwo amene amaopa Iye,

kuti ulemerero wake ukhale mʼdziko lathu.

10Chikondi ndi kukhulupirika zimakumana pamodzi;

chilungamo ndi mtendere zimapsompsonana.

11Kukhulupirika kumatumphuka kuchokera ku dziko lapansi,

ndipo chilungamo chimayangʼana pansi kuchokera kumwamba.

12Ndithu Yehova adzapereka chimene chili chabwino,

ndipo dziko lathu lidzapereka zokolola zake.

13Wolungama amapita patsogolo pake

ndi kukonza njira za mapazi ake.

Korean Living Bible

시편 85:1-13

나라의 번영을 위한 기도

(고라 자손의 시. 성가대 지휘자를 따라 부른 노래)

1여호와여,

주께서 이 땅을 축복하셔서

다시 이스라엘을

번영하게 하셨습니다.

2주께서는 주의 백성의 죄를

용서하시고

그들의 모든 허물을 덮어 주셨으며

3주의 모든 분노를 거두셨습니다.

4우리 구원의 하나님이시여,

우리를 다시 회복시켜 주시고

우리에 대한 주의 분노를 그치소서.

5주께서 우리에게 영원히 노하시며

대대로 분노하시겠습니까?

6우리를 다시 살려 주소서.

그러면 주의 백성인 우리가

주를 찬양하며 기뻐하겠습니다.

7여호와여, 우리에게

주의 한결같은 사랑을 보이시고

우리에게 주의 구원을

베풀어 주소서.

8나는 여호와 하나님의

말씀을 들으리라.

그는 자기 백성인 성도들이

어리석은 길로

되돌아가지 않는다면

그들에게 평안을 약속하실 것이다.

9그를 두려워하는 자에게

구원이 가까우니

우리 땅에 그의 영광이 있으리라.

10사랑과 85:10 또는 ‘진리가’성실이 함께 만나고

의와 평화가 서로 입맞추니

11성실은 땅에서 솟아오르고

의는 하늘에서 굽어살피는구나.

12여호와께서 좋은 것을 주시리니

우리 땅이 농산물을 내리라.

13의가 여호와 앞에서 행하며

그를 위해 길을 예비하리라.