Masalimo 60 – CCL & JCB

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Masalimo 60:1-12

Salimo 60

Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Potsata mayimbidwe a “Kakombo wa Pangano.” Mikitamu ya Davide yophunzitsira. Pamene anamenyana ndi Mesopotamiya ndi Aramu-Zoba, ndi pamene Yowabu anabwerera ndi kukantha Aedomu 12,000 mʼChigwa cha Mchere.

1Inu Mulungu mwatikanatu ife, ndipo mwatiwonongera otiteteza.

Inu mwatikwiyira, tsopano tibwezeretseni mwakale!

2Inu mwagwedeza dziko ndipo mwalingʼamba,

konzani mingʼalu yake pakuti ikugwedezeka kwambiri.

3Inu mwaonetsa anthu anu nthawi za mavuto;

inu mwatipatsa vinyo amene watichititsa kudzandira.

4Koma kwa iwo amene amaopa Inu, Inu mwakweza mbendera

kuti tisonkhanireko pothawa uta.

5Tipulumutseni ndi kutithandiza ndi dzanja lanu lamanja,

kuti iwo amene mumawakonda apulumutsidwe.

6Mulungu wayankhula kuchokera ku malo ake opatulika:

“Mwakupambana ndidzagawa Sekemu

ndipo ndidzayeza malire a chigwa cha Sukoti.

7Giliyadi ndi wanga, Manase ndi wanganso;

Efereimu ndi chipewa changa chodzitetezera,

Yuda ndi ndodo yanga yaufumu

8Mowabu ndi mbale yanga yosambira,

pa Edomu ndidzaponyapo nsapato yanga,

pa Filisitiya ndidzafuwula mwakupambana.”

9Adzandifikitse ndani ku mzinda wotetezedwa?

Ndani adzanditsogolera ku Edomu?

10Kodi si Inu Mulungu, Inu amene mwatikana ife

ndipo simutuluka pamodzi ndi magulu athu ankhondo.

11Tipatseni chithandizo kuti tilimbane ndi mdani wathu,

pakuti thandizo lochokera kwa munthu ndi lopanda phindu.

12Chifukwa cha Mulungu, ife tidzapeza chipambano

ndipo tidzapondaponda adani athu.

Japanese Contemporary Bible

詩篇 60:1-12

60

ダビデがシリヤ(アラム)と戦い、戦況がまだはっきりしていなかったとき、司令官ヨアブが塩の谷でエドム人一万二千人を打ち殺した。その時のダビデの作。

1ああ神よ。

あなたは私たちを拒み、その守りをもくずされました。

御怒りにふれて、私たちは見捨てられたのです。

主よ、もう一度、情けをかけてください。

2あなたはこの国を恐怖で震撼させ、引き裂かれました。

主よ、深みまで揺るがされたこの地を今、

回復してください。

3さんざんに打ちのめされて、

私たちの足はよろめいています。

4-5しかし、あなたはこんな私たちを

奮起させるための旗を下さいました。

真理を愛する人々が、この旗のもとに集うためです。

そうしてこそ、あなたは愛する国民に

解放をもたらしてくださるのです。

どうか、力に満ちた右の手をふるって、

私たちを救い出してください。

6-7神は、ご自分の名誉にかけて

救援を約束してくださいました。

私は大いに喜びました。

神はこう宣言なさいます。

「シェケム、スコテ、ギルアデ、マナセは、

依然としてわたしのものだ。

ユダからは継続して王が出、

エフライムからは勇士が誕生する。

8モアブはわたしの召使となり、

エドムは奴隷となる。

わたしはまた、ペリシテを攻め取って、

勝利の声を上げよう。」

9-10あの強固なエドムの町に、

この私を入城させてくださるのはどなたでしょう。

それは神です。

私たちを捨てて敵の手に渡された、その神です。

11主よ、どうか敵の攻撃から守ってください。

人の助けなど、あてになりません。

12神の助けがあれば、

私たちは強力な働きを進めることができます。

神が敵を踏みつけてくださるからです。