Masalimo 58 – CCL & NEN

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Masalimo 58:1-11

Salimo 58

Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Potsata mayimbidwe a “Musawononge.” Ndakatulo ya Davide.

1Kodi inu olamulira mumayankhuladi molungama?

Kodi mumaweruza mwachilungamo pakati pa anthu?

2Ayi, mʼmitima mwanu mumakonzekera zosalungama,

ndipo manja anu amatulutsa zachiwawa pa dziko lapansi.

3Ngakhale kuchokera tsiku lawo lobadwa oyipa amasochera;

kuchokera mʼmimba ya amayi awo, iwo ndi otayika ndipo amayankhula mabodza.

4Ululu wawo uli ngati ululu wa njoka,

ngati uja wa mphiri imene yatseka mʼmakutu mwake.

5Imene simva liwu la munthu wamatsenga,

ngakhale akhale wa luso lotani munthu wamatsengayo.

6Gululani mano mʼkamwa mwawo, Inu Mulungu,

Yehova khadzulani mano a mikango!

7Mulole kuti asowe ngati madzi oyenda

pamene iwo akoka uta mulole kuti mivi yawo ikhale yosathwa.

8Akhale ngati nkhono imene imasungunuka pamene ikuyenda;

ngati mwana wakufa asanabadwe, iwo asaone dzuwa.

9Miphika yanu isanagwire moto waminga ya mkandankhuku,

kaya iyo ndi yobiriwira kapena yowuma, oyipa adzachotsedwa.

10Olungama adzasangalala poona kubwezera chilango,

pamene adzasambitsa mapazi awo mʼmagazi a anthu oyipa.

11Ndipo anthu adzanena kuti,

“Zoonadi, olungama amalandirabe mphotho;

zoonadi kuli Mulungu amene amaweruza dziko lapansi.”

Kiswahili Contemporary Version (Neno: Bibilia Takatifu)

Zaburi 58:1-11

Zaburi 58

Mungu Kuwaadhibu Waovu

Kwa mwimbishaji. Mtindo wa “Usiharibu!” Utenzi wa Daudi.

1Enyi watawala, je, kweli mwanena kwa haki?

Je, mnahukumu kwa unyofu miongoni mwa watu?

258:2 Za 74:20; Isa 10:1; Mt 15:19; Lk 6:38La, mioyoni mwenu mnatunga udhalimu,

na mikono yenu hupima jeuri duniani.

358:3 Za 51:5Waovu ni wapotovu tangu kuzaliwa kwao,

toka tumboni mwa mama zao

ni wakaidi na husema uongo.

458:4 Hes 21:6; Za 140:4Sumu yao ni kama sumu ya nyoka,

kama ile ya fira ambaye ameziba masikio yake,

558:5 Za 81:11; Mhu 10:1; Yer 8:17ambaye hatasikia sauti ya kutumbuiza ya mwaguzi,

hata kama mganga angecheza kwa ustadi kiasi gani.

658:6 Ay 4:10; Za 3:7Ee Mungu, yavunje meno katika vinywa vyao;

Ee Bwana, vunja meno makali ya hao simba!

758:7 Law 26:36; Ay 11:16; Za 11:2; 57:4; 64:3Na watoweke kama maji yapitayo kwa kasi,

wavutapo pinde zao, mishale yao na iwe butu.

858:8 Isa 13:7; Ay 3:16Kama konokono ayeyukavyo akitembea,

kama mtoto aliyezaliwa akiwa mfu,

wasilione jua.

958:9 Za 118:12; Mhu 7:6; Ay 7:10; Mit 10:25Kabla vyungu vyenu havijapata moto wa kuni za miiba,

zikiwa mbichi au kavu,

waovu watakuwa

wamefagiliwa mbali.

1058:10 Ay 22:19; Kum 32:42; 32:35; Yer 11:20; Mit 10:11; Rum 12:17-21; Za 18:47; 7:9; 91:8; 68:23; Ufu 18:20Wenye haki watafurahi waonapo wakilipizwa kisasi,

watakapochovya nyayo zao katika damu ya waovu.

1158:11 Mwa 4:12, 13; 15:1; Za 128:2; Lk 6:23; Ufu 2:23; Rum 2:6-11; 14:12; Ay 34:11; Mhu 5:8; Yer 32:19; Eze 7:27Ndipo wanadamu watasema,

“Hakika utulivu wa wenye haki bado una thawabu,

hakika kuna Mungu ahukumuye dunia.”