Masalimo 150 – CCL & NEN

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Masalimo 150:1-6

Salimo 150

1Tamandani Yehova.

Tamandani Mulungu mʼmalo ake opatulika;

mutamandeni ku thambo lake lamphamvu.

2Mutamandeni chifukwa cha machitidwe ake amphamvu;

mutamandeni chifukwa cha ukulu wake wopambana.

3Mutamandeni poyimba malipenga,

mutamandeni ndi pangwe ndi zeze.

4Mutamandeni ndi matambolini ndi kuvina,

mutamandeni ndi zingwe ndi zitoliro.

5Mutamandeni ndi ziwaya zolira za malipenga,

mutamandeni ndi ziwaya zolira kwambiri.

6Chamoyo chilichonse chopuma chitamande Yehova.

Tamandani Yehova.

Kiswahili Contemporary Version (Neno: Bibilia Takatifu)

Zaburi 150:1-6

Zaburi 150

Msifuni Bwana Kwa Ukuu Wake

1150:1 Za 112:1; 73:17; 68:24-26; 102:19; 148:1Msifuni Bwana.

Msifuni Mungu katika patakatifu pake,

msifuni katika mbingu zake kuu.

2150:2 Kum 3:24; Kut 15:7Msifuni kwa matendo yake makuu,

msifuni kwa kadiri ya wingi wa ukuu wake.

3150:3 Hes 10:2; Za 57:8Msifuni kwa mvumo wa tarumbeta,

msifuni kwa kinubi na zeze,

4150:4 Kut 15:20; Za 45:8; Isa 38:20; Mwa 4:21msifuni kwa matari na kucheza,

msifuni kwa kinanda cha nyuzi na filimbi,

5150:5 2Sam 6:5msifuni kwa matoazi yaliayo,

msifuni kwa matoazi yavumayo sana.

6150:6 Za 103:22; Ufu 5:13Kila chenye pumzi na kimsifu Bwana.

Msifuni Bwana!