Masalimo 13 – CCL & CARS

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Masalimo 13:1-6

Salimo 13

Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Salimo la Davide.

1Mpaka liti Yehova? Kodi mudzandiyiwala mpaka kalekale?

Mpaka liti mudzandibisira nkhope yanu?

2Ndidzalimbana ndi maganizo anga

ndi kukhala ndi chisoni mu mtima mwanga tsiku lililonse mpaka liti?

Mpaka liti adani anga adzandipambana?

3Ndiyangʼaneni ndi kundiyankha, Inu Yehova Mulungu wanga.

Walitsani maso anga kuti ndingafe;

4mdani wanga adzati, “Ndamugonjetsa,”

ndipo adani anga adzakondwera pamene ine ndagwa.

5Koma ndikudalira chikondi chanu chosasinthika;

mtima wanga umakondwera ndi chipulumutso chanu.

6Ine ndidzayimbira Yehova

pakuti wandichitira zokoma.

Священное Писание

Забур 13:1-7

Песнь 13

(Заб. 52)

Дирижёру хора. Песнь Давуда.

1Говорят безумцы в сердце своём:

«Нет Всевышнего».

Они развратились, гнусны их дела;

нет делающего добро.

2Вечный взирает с небес на людей,

чтобы увидеть, есть ли понимающий,

ищущий Всевышнего.

3Все отвернулись от Всевышнего,

все, как один, развратились;

нет делающего добро,

нет ни одного.

4Неужели не вразумятся делающие зло –

те, кто поедает Мой народ, как хлеб,

и Вечного не призывает?

5Там их охватит страх,

потому что Всевышний на стороне праведных.

6Вы осмеяли надежды нищих,

но прибежище их – Вечный.

7Да придёт с Сиона спасение Исраилу!

Когда Вечный восстановит Свой народ,

пусть ликуют потомки Якуба и радуется Исраил!