Masalimo 13 – CCL & BPH

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Masalimo 13:1-6

Salimo 13

Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Salimo la Davide.

1Mpaka liti Yehova? Kodi mudzandiyiwala mpaka kalekale?

Mpaka liti mudzandibisira nkhope yanu?

2Ndidzalimbana ndi maganizo anga

ndi kukhala ndi chisoni mu mtima mwanga tsiku lililonse mpaka liti?

Mpaka liti adani anga adzandipambana?

3Ndiyangʼaneni ndi kundiyankha, Inu Yehova Mulungu wanga.

Walitsani maso anga kuti ndingafe;

4mdani wanga adzati, “Ndamugonjetsa,”

ndipo adani anga adzakondwera pamene ine ndagwa.

5Koma ndikudalira chikondi chanu chosasinthika;

mtima wanga umakondwera ndi chipulumutso chanu.

6Ine ndidzayimbira Yehova

pakuti wandichitira zokoma.

Bibelen på hverdagsdansk

Salmernes Bog 13:1-6

Et fortvivlet menneskes bøn

1Til korlederen: En sang af David.

2Hvor længe vil du glemme mig, Herre?—For evigt?

Hvor længe skal jeg vente på din hjælp?

3Hvor længe skal jeg kæmpe med sjæleangst?

Mine dage og nætter er fyldt med frygt.

Hvor længe skal fjenden triumfere over mig?

4Min Herre og Gud, åh, hør min bøn,

grib ind og red mig fra døden.

5Lad ikke mine fjender gå af med sejren,

lad ikke mine uvenner glædes over min undergang.

6Jeg stoler på dig og din trofasthed.

Jeg vil juble, når jeg oplever din frelse.

Jeg vil prise dig, Herre, med sang,

for din underfulde godhed imod mig.