Salimo 121
Nyimbo yoyimba pokwera ku Yerusalemu.
1Ndikweza maso anga ku mapiri;
kodi thandizo langa limachokera kuti?
2Thandizo langa limachokera kwa Yehova,
wolenga kumwamba ndi dziko lapansi.
3Sadzalola kuti phazi lako literereke;
Iye amene amakusunga sadzawodzera.
4Taonani, Iye amene amasunga Israeli
sadzawodzera kapena kugona.
5Yehova ndiye amene amakusunga;
Yehova ndiye mthunzi wako ku dzanja lako lamanja.
6Dzuwa silidzakupweteka nthawi ya masana,
kapena mwezi nthawi ya usiku.
7Yehova adzakuteteza ku zoyipa zonse;
adzasunga moyo wako.
8Yehova adzayangʼanira kutuluka kwako ndi kulowa kwako;
kuyambira tsopano mpaka muyaya.
1Een bedevaartslied. Ik hef mijn ogen omhoog naar de bergen: “Vanwaar komt mijn hulp?” 2Mijn hulp komt van Jahweh, Die hemel en aarde heeft gemaakt! 3Neen, Hij laat uw voeten niet struikelen, Hij slaapt niet, uw Wachter; 4Neen, Hij sluimert noch dommelt, Israëls Beschermer! 5Jahweh is uw Behoeder, Uw schaduw aan uw rechterhand: 6Overdag zal de zon u niet hinderen, En de maan niet des nachts. 7Jahweh behoedt u voor iedere ramp, Hij is bezorgd voor uw leven; 8Jahweh waakt over uw komen en gaan Van nu af tot in eeuwigheid.