Ukulu wa Mordekai
1Mfumu Ahasiwero anakhometsa msonkho mʼdziko lake lonse mpaka ku zilumba zonse. 2Ndipo ntchito zonse zochitika ndi mphamvu zake komanso ndi zonse zofotokoza za ukulu wa Mordekai, kukwezedwa kwake ndi mfumu, kodi sizinalembedwe mʼbuku la mbiri ya mafumu a ku Mediya ndi Peresiya? 3Pakuti Mordekai Myuda uja anali wachiwiri wa mfumu Ahasiwero. Kwa Ayuda onse Mordekai anali munthu wamkulu ndipo ankamukonda chifukwa ankachitira zabwino mtundu wake ndi kufunira mtendere abale ake.
Mordokaj hedras och får stor makt
1Kung Xerxes tog ut skatt från hela landet inklusive de avlägsna kustprovinserna. 2Alla hans storverk och bedrifter och berättelsen om den storhet han gav Mordokaj finns nedtecknade i mediska och persiska kungars krönika. 3Juden Mordokaj hade den största makten i landet näst efter kung Xerxes själv, och han var mycket högt aktad bland judarna och älskad av sina landsmän. Han tänkte alltid på sitt folks bästa och talade alltid för sina landsmäns välfärd.