诗篇 115 – CCB & CCL

Chinese Contemporary Bible (Simplified)

诗篇 115:1-18

第 115 篇

上帝是独一真神

(平行经文:诗篇135:15-20

1耶和华啊,

不要将荣耀归于我们,

不要归于我们。

愿荣耀归于你的名,

因为你慈爱、信实!

2为何让列国说

“他们的上帝在哪里”?

3我们的上帝高居在天,

按自己的旨意行事。

4他们的神像不过是人用金银造的。

5它们有口不能言,有眼不能看,

6有耳不能听,有鼻不能闻,

7有手不能摸,有脚不能走,

有喉咙也不能发声。

8那些制造它们、信靠它们的人也会和它们一样。

9以色列人啊,要信靠耶和华!

祂是你们的帮助,

是你们的盾牌。

10亚伦家啊,要信靠耶和华!

祂是你们的帮助,

是你们的盾牌。

11敬畏耶和华的人啊,要信靠祂!

祂是你们的帮助,

是你们的盾牌。115:4-11 平行经文:诗篇135:15-20

12耶和华眷顾我们,赐福给我们。

祂要赐福给以色列人,

赐福给亚伦家。

13耶和华要赐福给一切敬畏祂的人,

不分尊贵卑贱。

14愿耶和华使你们和你们的后代人丁兴旺!

15愿创造天地的耶和华赐福给你们!

16高天属于耶和华,

但祂把大地赐给了世人。

17死人不能歌颂耶和华,

下到坟墓的人不能赞美祂。

18但我们要赞美耶和华,

从现在直到永远。

你们要赞美耶和华!

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Masalimo 115:1-18

Salimo 115

1Kwa ife ayi Yehova, kwa ife ayi

koma ulemerero ukhale pa dzina lanu,

chifukwa cha chikondi chanu chosasinthika ndiponso chifukwa cha kukhulupirika kwanu.

2Chifukwa chiyani anthu a mitundu ina akunena kuti,

“Mulungu wawo ali kuti?”

3Mulungu wathu ali kumwamba;

Iye amachita chilichonse chimene chimamukondweretsa.

4Koma mafano awo ndi siliva ndi golide,

opangidwa ndi manja a anthu.

5Pakamwa ali napo koma sayankhula,

maso ali nawo koma sapenya;

6makutu ali nawo koma samva,

mphuno ali nazo koma sanunkhiza;

7manja ali nawo koma akakhudza samva kanthu;

mapazi ali nawo koma sayenda;

kapena pakhosi pawo kutulutsa mawu.

8Anthu amene amapanga mafanowo adzafanana nawo,

chimodzimodzinso onse amene amadalira mafanowo.

9Inu Aisraeli, dalirani Yehova;

Iye ndiye thandizo lanu ndi chishango chanu.

10Iwe nyumba ya Aaroni, dalira Yehova;

Iye ndiye thandizo lako ndi chishango chako.

11Inu amene mumaopa Iye, dalirani Yehova;

Iye ndiye thandizo lanu ndi chishango chanu.

12Yehova watikumbukira ndipo adzatidalitsa:

adzadalitsa nyumba ya Israeli,

adzadalitsa nyumba ya Aaroni,

13adzadalitsa iwo amene amaopa Yehova;

aangʼono ndi aakulu omwe.

14Yehova akuwonjezereni madalitso;

inuyo pamodzi ndi ana anu.

15Mudalitsidwe ndi Yehova,

Wolenga kumwamba ndi dziko lapansi.

16Kumwamba ndi kwa Yehova,

koma dziko lapansi Iye walipereka kwa anthu.

17Si anthu akufa amene amatamanda Yehova,

amene amatsikira kuli chete;

18ndi ife amene timatamanda Yehova,

kuyambira tsopano mpaka muyaya.

Tamandani Yehova.