箴言 15 – CCB & CCL

Chinese Contemporary Bible (Simplified)

箴言 15:1-33

1温和的回答平息怒气,

粗暴的言词激起愤怒。

2智者的舌头传扬知识,

愚人的嘴巴吐露愚昧。

3耶和华的眼目无所不在,

善人和恶人都被祂鉴察。

4温和的言词带来生命,

乖谬的话语伤透人心。

5愚人蔑视父亲的管教,

接受责备的才算明智。

6义人家中财富充足,

恶人得利惹来祸患。

7智者的嘴传扬知识,

愚人的心并非如此。

8耶和华憎恨恶人的祭物,

悦纳正直人的祈祷。

9耶和华憎恨恶人的行径,

喜爱追求公义的人。

10背离正道,必遭严惩;

厌恶责备,必致死亡。

11阴间和冥府15:11 冥府”希伯来文是“亚巴顿”,参考启示录9:11在耶和华面前尚且无法隐藏,

何况世人的心思呢!

12嘲讽者不爱听责备,

也不愿请教智者。

13心中喜乐,容光焕发;

心里悲伤,精神颓丧。

14哲士渴慕知识,

愚人安于愚昧。

15困苦人天天受煎熬,

乐观者常常有喜乐。

16财物虽少但敬畏耶和华,

胜过家财万贯却充满烦恼。

17粗茶淡饭但彼此相爱,

胜过美酒佳肴却互相憎恨。

18脾气暴躁,惹起争端;

忍耐克制,平息纠纷。

19懒惰人的路布满荆棘,

正直人的道平坦宽阔。

20智慧之子使父亲欢喜,

愚昧的人却藐视母亲。

21无知者以愚昧为乐,

明哲人遵循正道。

22独断专行,计划失败;

集思广益,事无不成。

23应对得体,心中愉快;

言语合宜,何等美好!

24智者循生命之路上升,

以免坠入阴间。

25耶和华拆毁傲慢人的房屋,

祂使寡妇的地界完整无损。

26耶和华憎恨恶人的意念,

喜爱纯洁的言语。

27贪爱财富,自害己家;

厌恶贿赂,安然存活。

28义人三思而后答,

恶人张口吐恶言。

29耶和华远离恶人,

却听义人的祷告。

30笑颜令人心喜,

喜讯滋润骨头。

31倾听生命的训诫,

使人与智者同列。

32不受管教就是轻看自己,

听从责备才能得到智慧。

33敬畏耶和华使人得智慧,

学会谦卑后才能得尊荣。

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Miyambo 15:1-33

1Kuyankha kofatsa kumathetsa mkwiyo,

koma mawu ozaza amautsa ukali.

2Munthu wanzeru amayankhula zinthu za nzeru,

koma pakamwa pa zitsiru pamatulutsa za uchitsiru.

3Maso a Yehova ali ponseponse,

amayangʼana pa oyipa ndi abwino omwe.

4Kuyankhula kodekha kuli ngati mtengo wopatsa moyo,

koma kuyankhula kopotoka kumapweteka mtima.

5Chitsiru chimanyoza mwambo wa abambo ake,

koma wochenjera amasamala chidzudzulo.

6Munthu wolungama amakhala ndi chuma chambiri,

zimene woyipa amapindula nazo zimamugwetsa mʼmavuto.

7Pakamwa pa anthu anzeru pamafalitsa nzeru;

koma mitima ya zitsiru sitero.

8Nsembe za anthu oyipa zimamunyansa Yehova,

koma amakondwera ndi pemphero la anthu owona mtima.

9Ntchito za anthu oyipa zimamunyansa Yehova

koma amakonda amene amafunafuna chilungamo.

10Amene amasiya njira yabwino adzalangidwa koopsa.

Odana ndi chidzudzulo adzafa.

11Manda ndi chiwonongeko ndi zosabisika pamaso pa Yehova,

nanji mitima ya anthu!

12Wonyoza sakonda kudzudzulidwa;

iye sapita kwa anthu anzeru.

13Mtima wokondwa umachititsa nkhope kukhala yachimwemwe,

koma mtima wosweka umawawitsa moyo.

14Mtima wa munthu wozindikira zinthu umafunafuna nzeru,

koma pakamwa pa zitsiru pamadya uchitsiru wawo.

15Munthu woponderezedwa masiku ake onse amakhala oyipa,

koma mtima wachimwemwe umakhala pa chisangalalo nthawi zonse.

16Kuli bwino kukhala ndi zinthu pangʼono nʼkumaopa Yehova,

kusiyana ndi kukhala ndi chuma chambiri uli pamavuto.

17Kuli bwino kudyera ndiwo zamasamba pamene pali chikondi,

kusiyana ndi kudyera nyama yangʼombe yonenepa pamene pali udani.

18Munthu wopsa mtima msanga amayambitsa mikangano,

koma munthu woleza mtima amathetsa ndewu.

19Njira ya munthu waulesi ndi yowirira ndi mtengo waminga,

koma njira ya munthu wolungama ili ngati msewu waukulu.

20Mwana wanzeru amakondweretsa abambo ake,

koma mwana wopusa amanyoza amayi ake.

21Uchitsiru umakondweretsa munthu wopanda nzeru,

koma munthu womvetsa zinthu amayenda mowongoka.

22Popanda uphungu zolinga zako munthu zimalephereka,

koma pakakhala aphungu ambiri zolinga zimatheka.

23Munthu amakondwera ndi kuyankha koyenera,

ndipo mawu onena pa nthawi yake ndi okoma.

24Munthu wanzeru amatsata njira yopita ku moyo

kuti apewe malo okhala anthu akufa.

25Yehova amapasula nyumba ya munthu wonyada

koma amasamalira malo a mkazi wamasiye.

26Maganizo a anthu oyipa amamunyansa Yehova,

koma mawu a anthu oyera mtima amamusangalatsa.

27Munthu wofuna phindu mwachinyengo amavutitsa banja lake,

koma wodana ndi ziphuphu adzakhala ndi moyo.

28Munthu wolungama amaganizira za mmene ayankhire,

koma pakamwa pa munthu woyipa pamatulutsa mawu oyipa.

29Yehova amakhala kutali ndi anthu oyipa,

koma amamva pemphero la anthu olungama.

30Kuwala kwa maso kumasangalatsa mtima

ndipo uthenga wabwino umalimbitsa munthu.

31Womvera mawu a chidzudzulo amene apatsa moyo

adzakhala pakati pa anthu anzeru.

32Amene amanyoza mwambo amadzinyoza yekha,

koma womvera mawu a chidzudzulo amapeza nzeru zomvetsa zinthu.

33Kuopa Yehova kumaphunzitsa munthu nzeru,

ndipo kudzichepetsa ndi ulemu chili patsogolo ndi kudzichepetsa.