Nnwom 98 – ASCB & CCL

Asante Twi Contemporary Bible

Nnwom 98:1-9

Dwom 98

Dwom.

1Monto dwom foforɔ mma Awurade,

ɛfiri sɛ wayɛ anwanwadeɛ bebree;

ne nsa nifa ne ne basa kronkron no

anya nkwagyeɛ ama no.

2Awurade ama wɔahunu ne nkwagyeɛ

na wada ne tenenee adi akyerɛ amanaman no.

3Wakae nʼadɔeɛ

ne ne nokorɛ a ɔdi akyerɛ Israelfoɔ;

asase ano nyinaa ahunu

yɛn Onyankopɔn nkwagyeɛ.

4Asase nyinaa mommɔ ose mma Awurade,

momfa nnwontoɔ nni ahurisie;

5Momfa sankuo nto dwom mma Awurade,

sankuo ne nnwontoɔ nnyegyeɛ,

6momfa totorobɛnto ne nnwennini mmɛn,

nteam ahosɛpɛ so wɔ Awurade, yɛn ɔhene no anim.

7Ɛpo ne abɔdeɛ a ɛwɔ mu nyinaa monworo so;

asase ne wɔn a wɔte soɔ nyinaa.

8Momma nsubɔntene mmɔ wɔn nsam,

mmepɔ nka mmom nto ahurisie dwom;

9ma wɔnto dwom wɔ Awurade anim,

ɛfiri sɛ ɔreba abɛbu ewiase atɛn.

Ɔde tenenee bɛbu ewiase atɛn

na ɔde pɛpɛyɛ abu nnipa atɛn.

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Masalimo 98:1-9

Salimo 98

Salimo.

1Imbirani Yehova nyimbo yatsopano,

pakuti Iyeyo wachita zinthu zodabwitsa;

dzanja lake lamanja ndi mkono wake woyera

zamuchitira chipulumutso.

2Yehova waonetsa chipulumutso chake

ndipo waulula chilungamo chake kwa anthu a mitundu ina.

3Iye wakumbukira chikondi chake

ndi kukhulupirika kwake pa Aisraeli;

malekezero onse a dziko lapansi aona

chipulumutso cha Mulungu wathu.

4Fuwulani mwachimwemwe kwa Yehova, dziko lonse lapansi,

muyimbireni nyimbo mofuwula ndi mokondwera.

5Imbirani Yehova nyimbo ndi zeze,

ndi zeze ndi mawu a kuyimba,

6ndi malipenga ndi kuliza kwa nyanga ya nkhosa yayimuna

fuwulani mwachimwemwe pamaso pa Yehova Mfumu.

7Nyanja ikokome pamodzi ndi zonse zili mʼmenemo,

dziko lonse ndi onse amene amakhala mʼmenemo.

8Mitsinje iwombe mʼmanja mwawo,

mapiri ayimbe pamodzi mwachimwemwe;

9izo ziyimbe pamaso pa Yehova,

pakuti Iye akubwera kudzaweruza dziko lapansi.

Adzaweruza dziko lonse mwachilungamo,

ndi mitundu ya anthu mosakondera.