Dwom 110
Dawid dwom.
1Awurade ka kyerɛɛ me Wura sɛ,
“Tena me nifa so
kɔsi sɛ mede wʼatamfoɔ
bɛyɛ wo nan ntiasoɔ.”
2Awurade bɛtrɛ wʼahempoma denden mu afiri Sion;
na wobɛdi ɔhene wɔ wʼatamfoɔ so.
3Wʼakodɔm bɛyi wɔn akoma mu
ɛda a wobɛkɔ sa.
Tumi kronkron bɛyɛ wʼaduradeɛ
na wo mmabunu bɛba wo nkyɛn
sɛdeɛ bosuo gugu anɔpahema.
4Awurade aka ntam
na ɔrensesa nʼadwene:
“Woyɛ daapem ɔsɔfoɔ
te sɛ Melkisedek sɛso.”
5Awurade wɔ wo nifa so;
ɔbɛdwerɛ ahemfo wɔ nʼabufuhyeɛ da no.
6Ɔbɛbu amanaman atɛn aboaboa afunu ano;
na wadwerɛ sodifoɔ a wɔwɔ asase so nyinaa.
7Ɔbɛnom asuwa a ɛda ɛkwan nkyɛn mu nsuo
enti ɔbɛdi nkonim.
Ɔhene no bɛnom asuwa a ɛda kwankyɛn mu nsuo,
na wanya ahoɔden, na wagyina nkonimdie mu.
Salimo 110
Salimo la Davide.
1Yehova akuwuza Mbuye wanga kuti,
“Khala ku dzanja langa lamanja
mpaka nditasandutsa adani ako
kukhala chopondapo mapazi ako.”
2Yehova adzakuza ndodo yamphamvu ya ufumu wako kuchokera mʼZiyoni;
udzalamulira pakati pa adani ako.
3Ankhondo ako adzakhala odzipereka
pa tsiku lako la nkhondo.
Atavala chiyero chaulemerero,
kuchokera mʼmimba ya mʼbandakucha,
udzalandira mame a unyamata wako.
4Yehova walumbira
ndipo sadzasintha maganizo ake:
“Ndiwe wansembe mpaka muyaya
monga mwa unsembe wa Melikizedeki.”
5Ambuye ali kudzanja lako lamanja;
Iye adzaponda mafumu pa tsiku la ukali wake.
6Adzaweruza anthu a mitundu ina,
adzadzaza dziko lapansi ndi mitembo ndipo adzaphwanya olamulira a pa dziko lonse lapansi.
7Iye adzamwa mu mtsinje wa mʼmbali mwa njira;
choncho adzaweramutsa mutu wake.