Nnwom Mu Dwom 6 – AKCB & CCL

Akuapem Twi Contemporary Bible

Nnwom Mu Dwom 6:1-13

Nnamfonom:

1Ɛhe na wo dɔfo no kɔ

mmea ahoɔfɛfo mu ahoɔfɛ?

Ɛhe na wo dɔfo man fae,

na yɛne wo nkɔhwehwɛ no?

Ababaa:

2Me dɔfo kɔ ne turo mu,

faako a woduadua nnua ahorow,

okokyinkyin turo no mu

akɔboaboa sukooko ano.

3Me dɔfo yɛ me de, na me nso meyɛ ne de;

okyinkyin sukooko no mu.

Aberante:

4Me dɔfo, wo ho yɛ fɛ te sɛ Tirsa,6.4 Tirsa yɛ Kanaan tete kurow bi a Yeroboam de yɛɛ nʼahenkurow wɔ afe 930 AWK (ansa na wɔrewo Kristo) kosi afe 909 AWK wɔ atifi fam ahemman mu.

wʼahoɔfɛ te sɛ Yerusalem,

wusi pi te sɛ asraafo a wɔretu frankaa.

5Nhwɛ me saa;

wobunkam me so.

Wo ti nwi te sɛ mpapokuw a

wɔresian afi Gilead.

6Wo se te sɛ nguankuw a wɔatwitwa wɔn ho nwi foforo,

a wofi aguaree.

Baako mpo nyeraa ɛ.

7Wʼasontɔre a ɛhyɛ wo nkataanim mu

te sɛ ntunkum aduaba fa.

8Ebia na ɔyerenom yɛ aduosia,

mpenanom bɛyɛ aduɔwɔtwe,

ne mmabaa dodow a wontumi nkan wɔn;

9nanso mʼaborɔnoma a ne ho nni asɛm yɛ sononko;

ɔno nko ara ne ne na babea,

ɔno na nea ɔwoo no no pɛ nʼasɛm.

Mmabaa huu no no, wɔfrɛɛ no nhyira;

ahemmea ne mpenanom kamfoo no.

Nnamfonom:

10Hena na wapue sɛ ahemadakye yi,

ɔyɛ frɔmfrɔm sɛ ɔsram, na ɔhyerɛn sɛ owia,

nʼanuonyam te sɛ nsoromma a wɔsa so.

Aberante:

11Misian kɔɔ nnuaba pɔw mu hɔ

sɛ merekɔhwehwɛ afifide foforo a ɛwɔ obon no mu,

sɛ bobe no agu nhwiren,

anaasɛ ntunkum no ayɛ frɔmfrɔm.

12Mʼani baa me ho so no

na mʼadwene de me abesi me nkurɔfo adehye nteaseɛnam so.

Nnamfonom:

13San wʼakyi, san wʼakyi, Sulamit babea;

San bra, san bra ma yɛnhwɛ wo!

Aberante:

Adɛn nti na ɛsɛ sɛ mohwɛ Sulamit abeawa

sɛnea mohwɛ Mahanaim asaw no?

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Nyimbo ya Solomoni 6:1-13

Abwenzi

1Iwe wokongola kuposa akazi onsewa,

kodi wokondedwa wakoyo wapita kuti?

Kodi wokondedwa wakoyo wakhotera njira iti

kuti timufunefune pamodzi ndi iwe?

Mkazi

2Wachikondi wanga watsikira ku munda kwake,

ku timinda ta zokometsera zakudya,

akukadyetsa ziweto zake ku minda,

ndiponso akuthyola maluwa okongola.

3Wokondedwa wangayo ndine wake ndipo iyeyo ndi wangawanga;

amadyetsa ziweto zake pakati pa maluwa okongola.

Mwamuna

4Ndiwe wokongola, bwenzi langa, ngati Tiriza,

wokongola kwambiri ngati Yerusalemu,

ndiwe woopsa ngati gulu lankhondo lonyamula mbendera.

5Usandipenyetsetse;

pakuti maso ako amanditenga mtima.

Tsitsi lako lili ngati gulu la mbuzi

zikutsetsereka kuchokera ku Giliyadi.

6Mano ako ali ngati gulu la nkhosa

zimene zikubwera kuchokera kokazisambitsa,

iliyonse ili ndi ana amapasa,

palibe imene ili yokha.

7Kukhalira kumbuyo kwa nsalu yako yophimba kumutu,

masaya ako ali ngati mabandu a makangadza.

8Ngakhale patakhala akazi a mfumu 60,

ndi azikazi 80,

ndi anamwali osawerengeka;

9koma nkhunda yanga, wangwiro wanga ndi wosiyana ndi wina aliyense;

mwana wamkazi yekhayo wa amayi ake,

mwana wapamtima wa amene anamubereka.

Anamwali anamuona ndipo anamutcha wodala;

akazi a mfumu ndi azikazi anamutamanda.

Abwenzi

10Ndani uyu akuoneka ngati mʼbandakucha,

wokongola ngati mwezi, wowala ngati dzuwa,

wochititsa mantha ngati gulu la ankhondo mbendera zili mʼmanja?

Mwamuna

11Ndinatsikira ku munda wa mitengo ya alimondi

kukayangʼana zomera zatsopano ku chigwa,

kukaona ngati mpesa waphukira

kapena ngati makangadza ali ndi maluwa.

12Ndisanazindikire kanthu,

ndinakhala ngati ndikulota kuti ndili mʼgaleta pambali pa mfumu yanga.

Abwenzi

13Bwerera, bwerera iwe namwali wa ku Sulami;

bwerera, bwerera kuti ife tidzakupenyetsetse iwe!

Mwamuna

Chifukwa chiyani mukufuna kudzapenyetsetsa ine mwana wamkazi wa ku Sulami,

pamene ndikuvina pakati pa magulu awiri?