บรรพ 1
สดุดี 1—41
สดุดี 1
1ความสุขมีแก่คนเหล่านั้นที่ไม่เดินตามรอยเท้าของคนชั่ว
หรือยืนอยู่ในทางของคนบาป
หรือนั่งอยู่ในที่นั่งของคนชอบเยาะเย้ย
2แต่พวกเขาปีติยินดีในบทบัญญัติขององค์พระผู้เป็นเจ้า
และใคร่ครวญบทบัญญัตินั้นทั้งกลางวันและกลางคืน
3พวกเขาเป็นเหมือนต้นไม้ที่ปลูกไว้ริมธารน้ำ
ซึ่งออกผลตามฤดูกาล
และใบก็ไม่เหี่ยวแห้ง
ทุกสิ่งที่พวกเขาทำก็เจริญรุ่งเรือง
4ส่วนคนชั่วไม่เป็นเช่นนั้น!
เขาเป็นเหมือนแกลบ
ซึ่งลมพัดปลิวฟุ้งไป
5ดังนั้นคนชั่วจะถูกตัดสินโทษเมื่อถึงวันพิพากษา
และคนบาปจะไม่อยู่ในที่ชุมนุมของผู้ชอบธรรม
6เพราะองค์พระผู้เป็นเจ้าทรงดูแลทางของคนชอบธรรม
แต่ทางของคนชั่วจะพินาศ
BUKU LOYAMBA
Masalimo 1–41
Salimo 1
1Wodala munthu
amene satsatira uphungu wa anthu ochimwa,
kapena kuyima mʼnjira ya anthu oyipa,
kapena kukhala mʼmagulu a anthu onyoza.
2Koma chikondwerero chake chili mʼmalamulo a Yehova
ndipo mʼmalamulo akewo amalingaliramo usana ndi usiku.
3Iye ali ngati mtengo wodzalidwa mʼmbali mwa mitsinje ya madzi,
umene umabereka zipatso zake pa nyengo yake
ndipo masamba ake safota.
Chilichonse chimene amachita amapindula nacho.
4Sizitero ndi anthu oyipa!
Iwo ali ngati mungu
umene umawuluzidwa ndi mphepo.
5Kotero anthu oyipa sadzatha kuyima pa chiweruzo,
kapena anthu ochimwa mu msonkhano wa anthu olungama.
6Pakuti Yehova amayangʼanira mayendedwe a anthu olungama,
koma mayendedwe a anthu oyipa adzawonongeka.