Salmos 126 – NVI-PT & CCL

Nova Versão Internacional

Salmos 126:1-6

Salmo 126

Cântico de Peregrinação.

1Quando o Senhor trouxe os cativos

de volta a Sião126.1 Ou trouxe restauração a Sião, foi como um sonho.

2Então a nossa boca encheu-se de riso

e a nossa língua de cantos de alegria.

Até nas outras nações se dizia:

“O Senhor fez coisas grandiosas por este povo”.

3Sim, coisas grandiosas fez o Senhor por nós,

por isso estamos alegres.

4Senhor, restaura-nos126.4 Ou traze nossos cativos de volta,

assim como enches o leito dos ribeiros no deserto126.4 Ou Neguebe.

5Aqueles que semeiam com lágrimas,

com cantos de alegria colherão.

6Aquele que sai chorando

enquanto lança a semente,

voltará com cantos de alegria,

trazendo os seus feixes.

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Masalimo 126:1-6

Salimo 126

Nyimbo yoyimba pokwera ku Yerusalemu.

1Yehova atabwezera akapolo ku Ziyoni,

tinali ngati amene akulota.

2Pakamwa pathu panadzaza ndi kuseka;

malilime athu ndi nyimbo zachimwemwe.

Pamenepo kunanenedwa pakati pa anthu kuti,

“Yehova wawachitira zinthu zazikulu.”

3Yehova watichitira zinthu zazikulu,

ndipo tadzazidwa ndi chimwemwe.

4Tibwezereni madalitso athu, Inu Yehova,

monga mitsinje ya ku Negevi.

5Iwo amene amafesa akulira,

adzakolola akuyimba nyimbo zachimwemwe.

6Iye amene amayendayenda nalira,

atanyamula mbewu yokafesa,

adzabwerera akuyimba nyimbo zachimwemwe,

atanyamula mitolo yake.