Псалми 67 – NSP & CCL

New Serbian Translation

Псалми 67:1-7

Псалам 67

Хоровођи, уз жичане инструменте. Псалам. Песма.

1Смиловао нам се Бог и благословио нас,

лицем својим обасјао нас; Села

2да би се на земљи знало за пут твој,

за спасење твоје у свим народима.

3Нек те хвале народи, о, Боже,

нек те хвале сви народи.

4Нека се радују и нек се веселе људи,

јер праведно судиш народима

и водиш људе на земљи. Села

5Нек те хвале народи, о, Боже,

нек те хвале сви народи.

6Земља рађа својим плодовима;

благословио нас Бог, Бог наш.

7Благословио нас Бог

да би га се бојали сви крајеви земље.

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Masalimo 67:1-7

Salimo 67

Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Pa zoyimbira za zingwe. Salimo.

1Yehova atikomere mtima ndi kutidalitsa,

achititse kuti nkhope yake itiwalire.

2Kuti njira zanu zidziwike pa dziko lapansi,

chipulumutso chanu pakati pa mitundu yonse.

3Mitundu ya anthu ikutamandeni Inu Mulungu;

mitundu yonse ya anthu ikutamandeni.

4Mitundu yonse ya anthu isangalale ndi kuyimba mwachimwemwe,

pakuti inu mumaweruza mitundu ya anthu mwachilungamo

ndi kutsogolera mitundu ya anthu a dziko lapansi.

5Mitundu ya anthu ikutamandeni Inu Mulungu;

mitundu yonse ya anthu ikutamandeni.

6Nthaka yabereka zokolola zake;

tidalitseni Mulungu wathu.

7Mulungu atidalitse

kuti pamenepo malekezero onse a dziko lapansi apembedze Iyeyo.