Псалам 54
Хоровођи, уз жичане инструменте. Давидова поучна песма, када су Зифејци дошли Саулу и рекли: „Не крије ли се Давид код нас?“
1Боже, именом ме својим спаси
и снагом ме својом ти одбрани.
2Боже, чуј молитву моју;
речи уста мојих послушај.
3Јер, против мене устају туђинци;
моју душу траже бездушници;
они Бога немају пред собом. Села
4Гле, Бог ми је помоћник;
Господ је међу онима што ми душу подупиру.
5Вратило се зло мрзитељу моме;
ти их сатри у верности својој.
6Радо ћу ти жртвовати;
хвалићу име твоје, Господе,
јер је добро.
7Јер оно ме је избавио из сваке невоље
и око ми победнички гледа противнике моје.
Salimo 54
Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Pa zoyimbira za zingwe. Ndakatulo ya Davide. Pamene anthu a ku Zifi anapita kwa Sauli ndipo anati, “Kodi Davide sakubisala pakati pathu.”
1Pulumutseni Inu Mulungu, mwa dzina lanu;
onetsani kuti ndine wosalakwa mwamphamvu yanu.
2Imvani pemphero langa, Inu Mulungu
mvetserani mawu a pakamwa panga.
3Alendo akundithira nkhondo;
anthu ankhanza akufunafuna moyo wanga,
anthu amene salabadira za Mulungu.
4Zoonadi Mulungu ndi thandizo langa;
Ambuye ndiye amene amandichirikiza ine.
5Lolani kuti choyipa chifike pa iwo amene amandichita chipongwe;
mwa kukhulupirika kwanu awonongeni.
6Ine ndidzapereka nsembe yaufulu kwa Inu;
ndidzatamanda dzina lanu, Inu Yehova,
pakuti ndi labwino.
7Pakuti Iyeyo wandipulumutsa ku masautso anga onse,
ndipo maso anga apenya kupambana kwa pa adani anga.