Псалми 43 – NSP & CCL

New Serbian Translation

Псалми 43:1-5

Псалам 43

1Досуди ми правду, Боже,

одбрани мој спор од безбожног света,

избави ме од човека подлог и неправедног.

2Јер ти си Бог мој, тврђава моја.

Зашто си ме одбацио?

Зашто идем около у жалости

под тлаком непријатеља мога?

3Пошаљи светлост и истину твоју да ме воде,

да ме доведу на свету гору твоју,

и до места где ти пребиваш.

4Приступићу тада к жртвенику Божијем,

к Богу радости и ужитка свог;

да те харфом хвалим, Боже, Боже мој.

5Зашто си ми клонула, душо моја,

зашто уздишеш у мени?

Богу се надај, јер опет ћу га славити,

Спаситеља и Бога свог.

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Masalimo 43:1-5

Salimo 43

1Onetsani kusalakwa kwanga Inu Mulungu;

ndipo mundinenere mlandu wanga kutsutsana ndi mtundu wosapembedza;

mundilanditse mʼmanja mwa achinyengo ndi anthu oyipa.

2Pajatu Inu Mulungu ndinu mphamvu zanga.

Nʼchifukwa chiyani mwandikana ine?

Nʼchifukwa chiyani ndiyenera kuyenda ndikulira,

woponderezedwa ndi mdani?

3Tumizani kuwunika kwanu ndi choonadi chanu

kuti zinditsogolere;

mulole kuti zindifikitse ku phiri lanu loyera,

kumalo kumene inu mumakhala.

4Ndipo ndidzapita ku guwa lansembe la Mulungu,

kwa Mulungu, chimwemwe changa ndi chikondwerero changa.

Ndidzakutamandani ndi zeze,

Inu Mulungu wanga.

5Nʼchifukwa chiyani uli ndi chisoni iwe moyo wanga?

Nʼchifukwa chiyani wakhumudwa iwe mʼkati mwanga?

Khulupirira Mulungu,

pakuti ndidzamutamandabe Iye,

Mpulumutsi wanga ndi Mulungu wanga.