Псалтирь 124 – NRT & CCL

New Russian Translation

Псалтирь 124:1-5

Псалом 124

1Песнь восхождения.

Те, кто надеется на Господа, – как гора Сион:

не поколеблются, пребудут вовеки.

2Как горы окружают Иерусалим,

так Господь окружает Свой народ

отныне и вовеки.

3Жезл нечестивых не останется

над землей праведных,

чтобы праведные не протянули

свои руки к беззаконию.

4Будь добр, Господи, к добрым

и к правым в сердцах своих.

5Но тех, кто следует кривыми путями,

да отвергнет Господь вместе со злодеями.

Мир Израилю!

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Masalimo 124:1-8

Salimo 124

Salimo la Davide. Nyimbo yoyimba pokwera ku Yerusalemu.

1Akanapanda kukhala mbali yathu Yehova,

anene tsono Israeli,

2akanapanda kukhala mbali yathu Yehova,

potiwukira anthuwo,

3iwo atatipsera mtima,

akanatimeza amoyo;

4chigumula chikanatimiza,

mtsinje ukanatikokolola,

5madzi a mkokomo

akanatikokolola.

6Atamandike Yehova,

amene sanalole kuti tikhale chakudya cha mano awo.

7Moyo wathu wawonjoka ngati mbalame

yokodwa mu msampha wa mlenje;

msampha wathyoka,

ndipo ife tapulumuka.

8Thandizo lathu lili mʼdzina la Yehova

wolenga kumwamba ndi dziko lapansi.